Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pakuti inu Yehova wa makamu, Mulungu wa Isiraeli, mwaululira ine mtumiki wanu kuti, ‘Ndidzakumangira nyumba.’*+ N’chifukwa chake ine mtumiki wanu ndalimba mtima kupemphera kwa inu pemphero lino.+

  • 1 Mafumu 2:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Tsopano m’dzina la Yehova Mulungu wamoyo,+ amene wandichititsa kukhazikika,+ amene wandiika pampando wachifumu wa Davide bambo anga,+ ndiponso amene anandipatsa mzere wa banja lachifumu+ monga ananenera,+ lero Adoniya aphedwa.”+

  • 1 Mbiri 17:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 ngati mmene anachitira kuchokera masiku amene ndinaika oweruza+ kuti azitsogolera anthu anga Aisiraeli. Ndipo ndidzatsitsa adani ako onse.+ Tsopano ndikukuuza kuti: ‘Kuwonjezera pamenepo, Yehova adzakumangira nyumba.’*+

  • 1 Mbiri 22:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iyeyo ndi amene adzamanga nyumba ya dzina langa.+ Adzakhala mwana+ wanga, ndipo ine ndidzakhala atate wake.+ Ndidzakhazikitsa mpando wake wachifumu+ pa Isiraeli ndipo sudzagwedezeka mpaka kalekale.’

  • Salimo 89:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 ‘Ndidzakhazikitsa mbewu yako mpaka kalekale,+

      Ndipo ndidzalimbitsa mpando wako wachifumu+ ku mibadwomibadwo.’” [Seʹlah.]

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena