Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 16:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ahabu anaimikanso mzati wopatulika,+ ndipo iye anachita zinthu zambiri zokwiyitsa+ Yehova Mulungu wa Isiraeli kuposa mafumu onse a Isiraeli amene anakhalapo iye asanakhale.

  • 1 Mafumu 21:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Choncho Ahabu analowa m’nyumba mwake ali wachisoni ndi wokhumudwa chifukwa cha mawu amene Naboti Myezereeli anamuuza, onena kuti: “Sindikupatsani cholowa cha makolo anga.” Ndiyeno anakagona pabedi lake n’kutembenukira kukhoma,+ ndipo sanadye chakudya.

  • 1 Mafumu 21:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 ndikubweretsera tsoka+ ndipo ndithu ndidzaseseratu nyumba yako,+ ndi kupha munthu aliyense wokodzera khoma+ wa m’banja la Ahabu, ngakhale anthu onyozeka ndi opanda pake mu Isiraeli.

  • 2 Mafumu 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ku Samariya+ kunali ana aamuna a Ahabu okwanira 70.+ Chotero Yehu analemba makalata n’kuwatumiza kwa atsogoleri+ a ku Yezereeli, kwa akuluakulu,+ ndi kwa anthu amene ankasamalira ana a Ahabu ku Samariya. M’makalatamo analembamo kuti:

  • 2 Mbiri 18:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yehosafati anakhala ndi chuma chambiri ndi ulemerero waukulu,+ koma anachita mgwirizano wa ukwati+ ndi Ahabu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena