-
Salimo 115:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Pakamwa ali napo koma salankhula,+
Maso ali nawo koma saona.+
-
Salimo 135:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Pakamwa ali napo koma salankhula.+
Maso ali nawo koma saona.+
-
Danieli 5:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Mwadzikweza pamaso pa Ambuye wakumwamba+ ndipo anthu akubweretserani ziwiya za m’nyumba yake.+ Inuyo, nduna zanu, adzakazi anu ndi akazi anu ena apambali mwamwera vinyo m’ziwiya zimenezi. Mwatamanda milungu wamba yasiliva, yagolide, yamkuwa, yachitsulo, yamitengo ndi yamiyala+ imene siona, kumva kapena kudziwa kalikonse.+ Koma Mulungu amene amasunga mpweya wanu+ ndi njira zanu zonse m’dzanja lake,+ simunamulemekeze.+
-
-
-
-
-