-
Yoswa 22:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Koma mukaonetsetse kuti mukusunga malamulo+ ndi Chilamulo chimene Mose mtumiki wa Yehova anakulamulirani. Mukachite zimenezi mwa kukonda Yehova Mulungu wanu,+ kuyenda m’njira zake zonse,+ kusunga malamulo ake,+ kum’mamatira,+ ndiponso kum’tumikira+ ndi mtima wanu wonse+ ndiponso moyo wanu wonse.”+
-