Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 11:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Atatero, anamuuza Yerobowamu kuti:

      “Tengapo zidutswa 10, pakuti Yehova Mulungu wa Isiraeli wati, ‘Ndikung’amba ufumuwu kuuchotsa m’manja mwa Solomo, ndipo iwe ndidzakupatsa mafuko 10.+

  • 1 Mafumu 12:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Yerobowamu+ mwana wa Nebati anamva zimenezi akadali ku Iguputo, (pajatu anathawa Mfumu Solomo n’kukakhala ku Iguputo),+

  • 1 Mafumu 12:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 M’mwezi wa 8, pa tsiku la 15 la mweziwo, Yerobowamu anachita chikondwerero chofanana ndi cha ku Yuda.+ Anachita chikondwererochi kuti apereke nsembe kwa ana a ng’ombe amene anawapanga, paguwa lansembe limene analimanga ku Beteli.+ M’malo okwezeka a ku Beteli amene anamanga, anaikako ansembe kuti azitumikira.

  • 1 Mafumu 14:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pa chifukwa chimenechi, ndibweretsa tsoka panyumba ya Yerobowamu. Ndithu ndidzapha munthu aliyense wokodzera khoma*+ wa m’nyumba ya Yerobowamu, ngakhale anthu onyozeka ndi opanda pake mu Isiraeli.+ Komanso ndidzaseseratu nyumba ya Yerobowamu,+ monga momwe munthu amasesera ndowe mpaka atakazitaya.+

  • 2 Mbiri 11:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Aleviwo anasiya malo awo odyetserako ziweto+ ndi madera awo+ n’kupita ku Yuda ndi ku Yerusalemu,+ chifukwa Yerobowamu+ ndi ana ake anachotsa+ Aleviwo pa udindo wokhala ansembe a Yehova.

  • 2 Mbiri 13:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Choncho Abiya anapita kukamenya nkhondoyo ndi gulu la amuna amphamvu ankhondo+ osankhidwa mwapadera okwanira 400,000. Yerobowamu nayenso anapita kukamenyana ndi Abiya ndipo anapita ndi asilikali 800,000. Amenewa anali amuna amphamvu ndi olimba mtima osankhidwa mwapadera, ndipo anakafola mwa dongosolo lomenyera nkhondo.+

  • 2 Mbiri 13:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Yerobowamu sanakhalenso ndi mphamvu+ m’masiku a Abiya, ndipo Yehova anamukantha+ moti anafa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena