Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 19:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Tsopano inu Yehova Mulungu wathu,+ chonde tipulumutseni+ m’manja mwake, kuti maufumu onse a padziko lapansi adziwe kuti inu Yehova, inu nokha ndiye Mulungu.”+

  • 2 Mbiri 32:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Tsopano musalole kuti Hezekiya akupusitseni+ kapena kukunyengererani+ chonchi ndipo musamukhulupirire, chifukwa palibe ufumu uliwonse kapena mulungu wa mtundu uliwonse wa anthu amene anatha kupulumutsa anthu akewo m’manja mwanga ndiponso m’manja mwa makolo anga. Ndiye mukuganiza kuti Mulungu wanu angakupulumutseni m’manja mwanga?’”+

  • Yobu 15:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Popeza amatambasula dzanja lake motsutsana ndi Mulungu,

      Ndipo amayesera kuti akhale wamkulu kuposa Wamphamvuyonse,+

  • Salimo 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mafumu a dziko lapansi aima pamalo awo,+

      Ndipo nduna zapamwamba zasonkhana pamodzi mogwirizana.+

      Atero kuti alimbane ndi Yehova+ komanso wodzozedwa wake.+

  • Yesaya 36:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndi mulungu uti pakati pa milungu yonse ya mayiko amenewa, amene walanditsa dziko lake m’manja mwanga,+ kuti Yehova athe kulanditsa Yerusalemu m’manja mwanga?”’”+

  • Yesaya 37:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Kodi ndani amene iwe wamutonza+ ndi kumulankhula monyoza?+

      Ndipo ndani amene iwe wam’kwezera mawu,+

      Ndi kum’kwezera maso ako m’mwamba?+

      Ndi Woyera wa Isiraeli!+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena