Salimo 51:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 51 Ndikomereni mtima inu Mulungu, malinga ndi kukoma mtima kwanu kosatha.+Malinga ndi kuchuluka kwa chifundo chanu, fafanizani zolakwa zanga.+ Salimo 85:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Inu Yehova, tisonyezeni kukoma mtima kwanu kosatha,+Ndipo tipatseni chipulumutso chanu.+ Salimo 90:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 M’mawa mutikhutiritse ndi kukoma mtima kwanu kosatha,+Kuti tifuule mokondwera ndi kuti tikhale osangalala masiku onse a moyo wathu.+ Salimo 106:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ndikumbukireni inu Yehova, ndipo ndisonyezeni kukoma mtima kumene mumasonyeza anthu anu.+Ndisamalireni ndi kundipulumutsa,+ Salimo 119:76 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 76 Kukoma mtima kwanu kosatha kundilimbikitse,+Monga mwa mawu anu kwa ine mtumiki wanu.+
51 Ndikomereni mtima inu Mulungu, malinga ndi kukoma mtima kwanu kosatha.+Malinga ndi kuchuluka kwa chifundo chanu, fafanizani zolakwa zanga.+
14 M’mawa mutikhutiritse ndi kukoma mtima kwanu kosatha,+Kuti tifuule mokondwera ndi kuti tikhale osangalala masiku onse a moyo wathu.+
4 Ndikumbukireni inu Yehova, ndipo ndisonyezeni kukoma mtima kumene mumasonyeza anthu anu.+Ndisamalireni ndi kundipulumutsa,+ Salimo 119:76 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 76 Kukoma mtima kwanu kosatha kundilimbikitse,+Monga mwa mawu anu kwa ine mtumiki wanu.+