Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 23:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Analinso kutumikira m’mawa ulionse+ pa nthawi yoimirira+ kuti athokoze+ ndi kutamanda+ Yehova. Analinso kuchita zimenezi madzulo.

  • Salimo 103:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Tamandani Yehova inu makamu ake onse,+

      Inu atumiki ake onse ochita chifuniro chake.+

  • Salimo 135:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Inu nyumba ya Isiraeli, tamandani Yehova.+

      Inu nyumba ya Aroni, tamandani Yehova.+

  • Luka 1:68
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 68 “Atamandike Yehova Mulungu wa Isiraeli,+ chifukwa wacheukira anthu ake+ ndi kuwapatsa chipulumutso.+

  • Yakobo 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pakuti lilime timatamanda nalo Yehova,+ amenenso ndi Atate,+ komanso ndi lilime lomwelo timatemberera+ anthu amene analengedwa “m’chifaniziro cha Mulungu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena