2 Samueli 8:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Davide anagonjetsanso Amowabu+ ndi kuwayeza ndi chingwe. Iye anawagoneka pansi kuti ayeze zingwe ziwiri ndi kuwapha, ndiponso chingwe chimodzi chathunthu n’kuwasiya amoyo.+ Choncho Amowabu anakhala atumiki a Davide+ ndipo anali kukhoma msonkho kwa iye.+ 2 Mafumu 21:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Ndithu ndidzayeza Yerusalemu ndi chingwe chimene ndinayezera+ Samariya,+ ndiponso ndidzamuyeza ndi thabwa lowongolera limene ndinayezera nyumba ya Ahabu.+ Yerusalemu ndidzam’pukuta+ mpaka kuyera mbee ngati mmene munthu amapukutira mbale yolowa mpaka kuyera mbee, n’kuitembenuza.+ Yesaya 28:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Kwa iwowo mawu a Yehova adzakhaladi “lamulo pa lamulo, lamulo pa lamulo, chingwe choyezera pachingwe choyezera, chingwe choyezera pachingwe choyezera,+ apa pang’ono, apo pang’ono,” kuti akagwe chagada n’kuthyoka, kukodwa ndi kugwidwa.+ Maliro 2:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Yehova waganiza zogwetsa mpanda+ wa mwana wamkazi wa Ziyoni.Watambasula chingwe choyezera.+ Sanabweze dzanja lake kuti lisabweretse chiwonongeko.+Walilitsa+ chiunda chomenyerapo nkhondo ndi mpanda. Zonsezi zatha mphamvu.
2 Davide anagonjetsanso Amowabu+ ndi kuwayeza ndi chingwe. Iye anawagoneka pansi kuti ayeze zingwe ziwiri ndi kuwapha, ndiponso chingwe chimodzi chathunthu n’kuwasiya amoyo.+ Choncho Amowabu anakhala atumiki a Davide+ ndipo anali kukhoma msonkho kwa iye.+
13 Ndithu ndidzayeza Yerusalemu ndi chingwe chimene ndinayezera+ Samariya,+ ndiponso ndidzamuyeza ndi thabwa lowongolera limene ndinayezera nyumba ya Ahabu.+ Yerusalemu ndidzam’pukuta+ mpaka kuyera mbee ngati mmene munthu amapukutira mbale yolowa mpaka kuyera mbee, n’kuitembenuza.+
13 Kwa iwowo mawu a Yehova adzakhaladi “lamulo pa lamulo, lamulo pa lamulo, chingwe choyezera pachingwe choyezera, chingwe choyezera pachingwe choyezera,+ apa pang’ono, apo pang’ono,” kuti akagwe chagada n’kuthyoka, kukodwa ndi kugwidwa.+
8 Yehova waganiza zogwetsa mpanda+ wa mwana wamkazi wa Ziyoni.Watambasula chingwe choyezera.+ Sanabweze dzanja lake kuti lisabweretse chiwonongeko.+Walilitsa+ chiunda chomenyerapo nkhondo ndi mpanda. Zonsezi zatha mphamvu.