-
2 Mafumu 18:32Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
32 kufikira ine nditabwera kudzakutengerani kudziko lofanana ndi dziko lanulo+ kuti mukhalebe ndi moyo osafa. Ndidzakutengerani kudziko la mbewu ndi la vinyo watsopano, dziko la mkate+ ndi minda ya mpesa,+ dziko la mitengo ya maolivi a mafuta ndiponso la uchi.+ Musamvere Hezekiya chifukwa akukunyengererani ndi mawu akuti, ‘Yehova atilanditsa.’+
-