Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Iwo andichititsa nsanje ndi milungu yachabe.+

      Andisautsa ndi mafano awo opanda pake.+

      Ndipo ine ndidzawachititsa nsanje ndi anthu achabe,+

      Ndidzawakhumudwitsa ndi mtundu wopusa.+

  • 2 Mafumu 17:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Iwo anapitiriza kuwotcha* pamoto+ ana awo aamuna ndi aakazi, kulosera+ ndi kuwombeza.*+ Anapitirizanso+ kuchita zoipa* pamaso pa Yehova ndi cholinga chomukwiyitsa.+

  • Nehemiya 9:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 “Koma iwo anakhala osamvera+ ndipo anakupandukirani.+ Anapitiriza kufulatira chilamulo chanu,+ ndipo anapha aneneri anu+ amene anali kuwalimbikitsa kuti abwerere kwa inu.+ Iwo anapitiriza kuchita zinthu zikuluzikulu zosakulemekezani.+

  • Yeremiya 7:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 ‘Kodi iwo akukhumudwitsa ine?’ watero Yehova.+ ‘Kodi iwo sakudzikhumudwitsa okha kuti achite manyazi pankhope zawo?’+

  • Yeremiya 32:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 “‘Ana a Isiraeli ndi ana a Yuda akhala akuchita zoipa pamaso panga kuyambira pa ubwana wawo.+ Ana a Isiraeli akundikhumudwitsa ndi ntchito za manja awo,’+ watero Yehova.

  • Yeremiya 44:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Koma inu simunamvere+ kapena kutchera khutu lanu kuti musiye kuchita zinthu zoipa zomwe ndi kupereka nsembe zautsi kwa milungu ina.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena