-
2 Mafumu 17:17Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
17 Iwo anapitiriza kuwotcha* pamoto+ ana awo aamuna ndi aakazi, kulosera+ ndi kuwombeza.*+ Anapitirizanso+ kuchita zoipa* pamaso pa Yehova ndi cholinga chomukwiyitsa.+
-