12 Ansembe+ ndi Alevi ambiri, omwe anali atsogoleri a nyumba za makolo awo,+ amuna okalamba amene anaona nyumba yoyambirira,+ anali kulira+ mokweza chifukwa cha kumangidwa kwa maziko+ a nyumbayo pamaso pawo, ndipo enanso ambiri anali kufuula mosangalala.+