Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 17:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Anasiya malamulo onse+ a Yehova Mulungu wawo n’kudzipangira zifaniziro ziwiri za ana a ng’ombe,+ zopangidwa ndi zitsulo zosungunula,+ komanso mzati wopatulika.+ Anayamba kugwadira khamu lonse la zinthu zakuthambo+ ndi kutumikira Baala.+

  • 2 Mbiri 28:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Koma anayenda m’njira za mafumu a Isiraeli,+ ndipo anafika mpaka popangira Abaala+ zifaniziro zopangidwa ndi zitsulo zosungunula.+

  • Yeremiya 7:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ana aamuna akutola nkhuni, abambo akuyatsa moto ndipo akazi akukanda ufa kuti apange makeke okapereka nsembe kwa ‘mfumukazi yakumwamba.’+ Ndipo akuthira pansi nsembe zachakumwa+ kwa milungu ina kuti andikhumudwitse.+

  • Yeremiya 19:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 ‘Nyumba za mu Yerusalemu ndi nyumba za mafumu a Yuda zidzakhala zodetsedwa ngati Tofeti.+ Zimenezi ndi nyumba zonse zimene pamadenga ake anali kufukizirapo nsembe zautsi kwa makamu akumwamba+ ndi kuthira nsembe zachakumwa kwa milungu ina.’”+

  • Yeremiya 44:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Yehova wa makamu, Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti, ‘Mawu awa akukhudza amuna inu ndi akazi anu.+ Akazi inu mumalankhula ndi pakamwa panu (ndipo anthu nonsenu mwakwaniritsa zonena zanu ndi manja anu) kuti: “Ife tidzakwaniritsa malonjezo athu+ akuti ‘tidzapereka nsembe zautsi kwa ‘mfumukazi yakumwamba’+ ndi kuti tidzapereka nsembe yachakumwa kwa iye.”+ Akazi inu mudzachitadi zimene mwalonjeza ndipo mudzakwaniritsadi malonjezo anu.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena