Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Nditaona kuti akuchita mantha, nthawi yomweyo ndinanyamuka ndi kuuza anthu olemekezeka,+ atsogoleri+ ndi anthu onse kuti: “Musachite nawo mantha+ anthu amenewa. Kumbukirani Yehova, Mulungu wamkulu+ ndi wochititsa mantha.+ Menyerani nkhondo abale anu,+ ana anu aamuna, ana anu aakazi, akazi anu ndi nyumba zanu.”

  • Nehemiya 9:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 “Tsopano Mulungu wathu, Mulungu wamkulu,+ wamphamvu+ ndi wochititsa mantha,+ wosunga pangano+ ndi kusonyeza kukoma mtima kosatha,+ musachepetse+ mavuto onse amene agwera ifeyo,+ mafumu athu,+ akalonga athu,+ ansembe athu,+ aneneri athu,+ makolo athu+ ndi anthu anu onse kuchokera masiku a mafumu a Asuri mpaka lero.+

  • Salimo 48:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Yehova ndi wamkulu ndi woyenera kutamandidwa kwambiri,+

      Mumzinda wa Mulungu wathu,+ m’phiri lake loyera.+

  • Salimo 145:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Yehova ndi wamkulu ndi woyenera kutamandidwa kwambiri,+

      Ndipo ukulu wake ndi wosasanthulika.+

  • Yeremiya 32:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Inu mumasonyeza anthu masauzande ambiri kukoma mtima kosatha.+ Mumabwezera zolakwa za abambo kwa ana awo.*+ Inu ndinu Mulungu woona, wamkulu+ ndi wamphamvu,+ ndipo dzina lanu+ ndinu Yehova wa makamu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena