Deuteronomo 30:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 “Ndiyeno zikadzachitika kuti mawu onsewa akwaniritsidwa pa inu, madalitso+ ndi matemberero+ amene ndakuikirani pamaso panu, ndipo mwakumbukira mawu amenewa mumtima mwanu+ muli pakati pa mitundu yonse kumene Yehova Mulungu wanu adzakubalalitsirani,+ Salimo 137:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 137 Tinakhala pansi+ m’mphepete mwa mitsinje ya ku Babulo,+Ndipo tinalira titakumbukira Ziyoni.+ Ezekieli 12:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Pakati pawo ndidzapulumutsapo amuna ochepa kuti asaphedwe ndi lupanga,+ njala, kapena miliri, n’cholinga chakuti akafotokoze za zinthu zawo zonse zonyansa+ pakati pa mitundu imene akakhaleko,+ ndipo adzadziwa kuti ine ndine Yehova.” Zekariya 10:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Ndidzawamwaza ngati mbewu pakati pa anthu a mitundu ina+ ndipo adzandikumbukira ali kumadera akutali.+ Iwowo ndi ana awo adzapezanso mphamvu ndipo adzabwerera.+
30 “Ndiyeno zikadzachitika kuti mawu onsewa akwaniritsidwa pa inu, madalitso+ ndi matemberero+ amene ndakuikirani pamaso panu, ndipo mwakumbukira mawu amenewa mumtima mwanu+ muli pakati pa mitundu yonse kumene Yehova Mulungu wanu adzakubalalitsirani,+
16 Pakati pawo ndidzapulumutsapo amuna ochepa kuti asaphedwe ndi lupanga,+ njala, kapena miliri, n’cholinga chakuti akafotokoze za zinthu zawo zonse zonyansa+ pakati pa mitundu imene akakhaleko,+ ndipo adzadziwa kuti ine ndine Yehova.”
9 Ndidzawamwaza ngati mbewu pakati pa anthu a mitundu ina+ ndipo adzandikumbukira ali kumadera akutali.+ Iwowo ndi ana awo adzapezanso mphamvu ndipo adzabwerera.+