Yesaya 43:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 “Inu ndinu mboni zanga,”+ akutero Yehova. “Ndinu mtumiki wanga amene ndakusankhani+ kuti mundidziwe+ ndi kundikhulupirira,+ komanso kuti mumvetse kuti ine sindinasinthe.+ Ine ndisanakhaleko kunalibe Mulungu amene anapangidwa,+ ndipo pambuyo panga palibenso wina.+ Yohane 17:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Atate, ine ndikufuna kuti amene mwandipatsawa adzakhale limodzi ndi ine kumene ine ndidzakhale,+ kuti adzaone ulemerero wanga umene inu mwandipatsa, chifukwa munandikonda musanayale maziko+ a dziko.+ Yuda 1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 1 Ine Yuda, kapolo wa Yesu Khristu koma m’bale wake wa Yakobo,+ ndikulembera oitanidwa+ okondedwa ndi Mulungu Atate, amene ali naye pa ubwenzi,+ amenenso asungidwa+ kuti akhale ogwirizana ndi Yesu Khristu.
10 “Inu ndinu mboni zanga,”+ akutero Yehova. “Ndinu mtumiki wanga amene ndakusankhani+ kuti mundidziwe+ ndi kundikhulupirira,+ komanso kuti mumvetse kuti ine sindinasinthe.+ Ine ndisanakhaleko kunalibe Mulungu amene anapangidwa,+ ndipo pambuyo panga palibenso wina.+
24 Atate, ine ndikufuna kuti amene mwandipatsawa adzakhale limodzi ndi ine kumene ine ndidzakhale,+ kuti adzaone ulemerero wanga umene inu mwandipatsa, chifukwa munandikonda musanayale maziko+ a dziko.+
1 Ine Yuda, kapolo wa Yesu Khristu koma m’bale wake wa Yakobo,+ ndikulembera oitanidwa+ okondedwa ndi Mulungu Atate, amene ali naye pa ubwenzi,+ amenenso asungidwa+ kuti akhale ogwirizana ndi Yesu Khristu.