Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 25
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 25:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 17:8; 19:17; 21:5
  • +De 16:18; 17:9
  • +Eks 23:6; 2Mb 19:6; Miy 17:15; 31:9; Yes 5:23

Deuteronomo 25:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 19:29; Lu 12:48
  • +Miy 10:13; 20:30; 26:3; Ahe 2:2

Deuteronomo 25:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ak 11:24

Deuteronomo 25:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 12:10; 1Ak 9:9; 1Ti 5:18

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    5/1/2012, tsa. 30

    5/1/1989, tsa. 17

Deuteronomo 25:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 38:8; Ru 4:5; Mko 12:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Baibulo la Dziko Latsopano (nwt), tsa. 2138

Deuteronomo 25:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 38:9; Ru 4:10, 14
  • +Nu 27:4; 2Sa 18:18

Deuteronomo 25:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ru 4:4

Deuteronomo 25:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ru 4:6

Deuteronomo 25:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ru 4:7
  • +Nu 12:14
  • +De 25:5

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    9/15/2004, tsa. 26

Deuteronomo 25:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 21:20; De 23:1

Deuteronomo 25:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 19:13, 21

Deuteronomo 25:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 11:1; 16:11; 20:10; Mik 6:11

Deuteronomo 25:14

Mawu a M'munsi

  • *

    Muyezo umodzi wa efa ndi wofanana ndi chitini cha malita 22.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 16:36; Le 19:36; Eze 45:10; Amo 8:5

Deuteronomo 25:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:40; 1Pe 3:10

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    8/2022, tsa. 27

Deuteronomo 25:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 19:35; Aro 9:14

Deuteronomo 25:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 17:8; Nu 24:20

Deuteronomo 25:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 15:16; Sl 36:1; Aro 3:18

Deuteronomo 25:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yos 22:4
  • +Eks 17:14; 1Sa 14:48; 15:3; 1Mb 4:43; Est 3:1; 7:10

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Tsanzirani, tsa. 144

    Nsanja ya Olonda,

    1/1/2012, tsa. 29

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 25:1De 17:8; 19:17; 21:5
Deut. 25:1De 16:18; 17:9
Deut. 25:1Eks 23:6; 2Mb 19:6; Miy 17:15; 31:9; Yes 5:23
Deut. 25:2Miy 19:29; Lu 12:48
Deut. 25:2Miy 10:13; 20:30; 26:3; Ahe 2:2
Deut. 25:32Ak 11:24
Deut. 25:4Miy 12:10; 1Ak 9:9; 1Ti 5:18
Deut. 25:5Ge 38:8; Ru 4:5; Mko 12:19
Deut. 25:6Ge 38:9; Ru 4:10, 14
Deut. 25:6Nu 27:4; 2Sa 18:18
Deut. 25:7Ru 4:4
Deut. 25:8Ru 4:6
Deut. 25:9Ru 4:7
Deut. 25:9Nu 12:14
Deut. 25:9De 25:5
Deut. 25:11Le 21:20; De 23:1
Deut. 25:12De 19:13, 21
Deut. 25:13Miy 11:1; 16:11; 20:10; Mik 6:11
Deut. 25:14Eks 16:36; Le 19:36; Eze 45:10; Amo 8:5
Deut. 25:15De 4:40; 1Pe 3:10
Deut. 25:16Le 19:35; Aro 9:14
Deut. 25:17Eks 17:8; Nu 24:20
Deut. 25:18Eks 15:16; Sl 36:1; Aro 3:18
Deut. 25:19Yos 22:4
Deut. 25:19Eks 17:14; 1Sa 14:48; 15:3; 1Mb 4:43; Est 3:1; 7:10
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 25:1-19

Deuteronomo

25 “Amuna akakangana+ n’kupita kwa oweruza,+ oweruzawo azigamula mlanduwo. Wolungama azimuweruza kuti ndi wolungama ndipo woipa azimuweruza kuti ndi woipa.+ 2 Ngati woipayo akuyenera kukwapulidwa,+ woweruza azilamula kuti woipayo amugoneke pansi, ndipo azim’kwapula+ pamaso pa woweruzayo. Azimukwapula zikoti zogwirizana ndi choipa chimene wachita. 3 Azimukwapula zikoti 40. Asapitirire pamenepo, kuopera kuti akapitiriza kumukwapula zikoti zambiri+ anganyazitse m’bale wako pamaso pako.

4 “Usamange ng’ombe pakamwa pamene ikupuntha mbewu.+

5 “Ngati amuna apachibale akukhala moyandikana, ndiyeno mmodzi n’kumwalira asanabereke mwana wamwamuna, mkazi wa womwalirayo asakwatiwe ndi mlendo wochokera m’banja lina. Mlamu wake apite kwa iye ndi kum’tenga kukhala mkazi wake, ndipo achite ukwati wa pachilamu.+ 6 Mwana woyamba amene mkaziyo angabereke, atenge dzina la mwamuna womwalira uja,+ kuti dzina la m’bale wake lisafafanizike mu Isiraeli.+

7 “Ngati mwamunayo sakufuna kutenga mkazi wamasiye wa m’bale wakeyo, mkaziyo azinyamuka ndi kupita kuchipata kwa akulu+ ndi kuwauza kuti, ‘M’bale wa mwamuna wanga wakana kusunga dzina la m’bale wake mu Isiraeli. Sanavomereze kuchita ukwati wa pachilamu ndi ine.’ 8 Pamenepo akulu a mzindawo amuitane ndi kulankhula naye. Iye aime pamaso pawo ndi kunena kuti, ‘Sindikufuna kutenga mkazi ameneyu.’+ 9 Zikatero mkazi wamasiyeyo aziyandikira m’bale wa mwamuna wakeyo akuluwo akuona ndipo azim’vula nsapato+ ndi kumulavulira kumaso.+ Pamenepo azinena kuti, ‘Izi ndiye zoyenera kuchitikira munthu wokana kumanga nyumba ya m’bale wake.’+ 10 Ndiyeno mu Isiraeli monse azidziwika ndi dzina lakuti, ‘Nyumba ya amene anavulidwa nsapato uja.’

11 “Amuna akamamenyana ndipo mkazi wa mmodzi mwa amunawo wabwera kudzalanditsa mwamuna wake m’manja mwa amene akumumenya, ndipo mkaziyo watambasula dzanja ndi kugwira mwamuna winayo kumaliseche,+ 12 uzidula dzanja la mkaziyo. Diso lako lisamve chisoni.+

13 “M’thumba lako, usakhale ndi miyezo iwiri yosiyana yoyezera kulemera kwa chinthu,+ usakhale ndi muyezo waukulu ndi wina waung’ono. 14 Usakhale ndi miyezo iwiri yosiyana ya efa*+ m’nyumba yako, usakhale ndi muyezo waukulu ndi muyezo waung’ono. 15 Muyezo wako woyezera kulemera kwa chinthu uzikhala wolondola ndi woyenera. Muyezo wako wa efa uzikhala wolondola ndi woyenera kuti masiku ako achuluke m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa.+ 16 Pakuti aliyense wochita zimenezi, aliyense wosachita chilungamo, n’ngonyansa kwa Yehova Mulungu wako.+

17 “Muzikumbukira zimene Aamaleki anakuchitirani panjira pamene munali kutuluka mu Iguputo.+ 18 Iwo anakumana nanu panjira ndi kupha anthu oyenda movutika m’gulu lanu amene anali kumbuyo. Iwo anachita izi pamene munali olefuka ndi otopa ndipo sanaope Mulungu.+ 19 Motero Yehova Mulungu wanu akakupumitsani kwa adani anu onse okuzungulirani, m’dziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kuti mulitenge kukhala cholowa chanu,+ mufafanize dzina la Amaleki pansi pa thambo.+ Musaiwale zimenezi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena