Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 24
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 24:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 19:3, 8
  • +Yer 3:8; Mt 5:31; Mko 10:4
  • +Mki 2:16; Mt 1:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    “Wotsatira Wanga,” ptsa. 104-105

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    12/2018, tsa. 11

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    8/2016, ptsa. 10-11

    Yesu—Ndi Njira, tsa. 222

    Nsanja ya Olonda,

    9/1/2008, tsa. 25

    8/15/1993, ptsa. 4-5

Deuteronomo 24:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 21:7; Mt 5:32; Mko 10:11

Deuteronomo 24:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 3:1

Deuteronomo 24:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 20:7; Lu 14:20
  • +Miy 5:18; Mla 9:9

Deuteronomo 24:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 22:26, 27

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/1/2014, tsa. 7

    9/15/2004, tsa. 26

Deuteronomo 24:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 40:15; Eks 21:16; 1Ti 1:10
  • +Ge 37:28
  • +De 19:19; 21:21

Deuteronomo 24:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 13:9; 14:2, 34
  • +Le 13:2, 15; 2Mb 26:20; Mki 2:7; Mko 1:44; Lu 17:14
  • +Sl 119:4

Deuteronomo 24:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 12:10, 15

Deuteronomo 24:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 15:8; Miy 3:27
  • +Yob 24:3

Deuteronomo 24:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yob 24:9, 10

Deuteronomo 24:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 22:26; Eze 18:7; 33:15
  • +Eks 22:27
  • +1Sa 25:14; Eze 33:15; 2Ak 9:13
  • +De 6:25; Sl 112:9; Da 4:27

Deuteronomo 24:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 25:40, 43; Miy 14:31; Mki 3:5

Deuteronomo 24:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 19:13; Yer 22:13; Mt 20:8
  • +Eks 22:23; Yob 34:28; Sl 25:1; 86:4; Miy 22:23; Yak 5:4
  • +Yak 4:17

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    1/2018, tsa. 32

Deuteronomo 24:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mb 25:4; Yer 31:30
  • +Eze 18:20

Deuteronomo 24:17

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu ake enieni, “mwana wamwamuna wopanda bambo.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 22:21; Eze 22:29
  • +Eks 22:22; Yes 1:23; Yer 5:28; Mki 3:5
  • +Eks 22:27; Yob 24:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    2/2019, tsa. 24

Deuteronomo 24:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:15; 15:15; 16:12

Deuteronomo 24:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 19:9
  • +Le 23:22; Ru 2:16; Sl 41:1
  • +De 15:10; Miy 11:24; 14:21; 19:17; Lu 6:38; 2Ak 9:6; 1Yo 3:17

Deuteronomo 24:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 19:10; De 26:13

Deuteronomo 24:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 13:3
  • +2Ak 8:8

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 24:1Mt 19:3, 8
Deut. 24:1Yer 3:8; Mt 5:31; Mko 10:4
Deut. 24:1Mki 2:16; Mt 1:19
Deut. 24:2Le 21:7; Mt 5:32; Mko 10:11
Deut. 24:4Yer 3:1
Deut. 24:5De 20:7; Lu 14:20
Deut. 24:5Miy 5:18; Mla 9:9
Deut. 24:6Eks 22:26, 27
Deut. 24:7Ge 40:15; Eks 21:16; 1Ti 1:10
Deut. 24:7Ge 37:28
Deut. 24:7De 19:19; 21:21
Deut. 24:8Le 13:9; 14:2, 34
Deut. 24:8Le 13:2, 15; 2Mb 26:20; Mki 2:7; Mko 1:44; Lu 17:14
Deut. 24:8Sl 119:4
Deut. 24:9Nu 12:10, 15
Deut. 24:10De 15:8; Miy 3:27
Deut. 24:10Yob 24:3
Deut. 24:12Yob 24:9, 10
Deut. 24:13Eks 22:26; Eze 18:7; 33:15
Deut. 24:13Eks 22:27
Deut. 24:131Sa 25:14; Eze 33:15; 2Ak 9:13
Deut. 24:13De 6:25; Sl 112:9; Da 4:27
Deut. 24:14Le 25:40, 43; Miy 14:31; Mki 3:5
Deut. 24:15Le 19:13; Yer 22:13; Mt 20:8
Deut. 24:15Eks 22:23; Yob 34:28; Sl 25:1; 86:4; Miy 22:23; Yak 5:4
Deut. 24:15Yak 4:17
Deut. 24:162Mb 25:4; Yer 31:30
Deut. 24:16Eze 18:20
Deut. 24:17Eks 22:21; Eze 22:29
Deut. 24:17Eks 22:22; Yes 1:23; Yer 5:28; Mki 3:5
Deut. 24:17Eks 22:27; Yob 24:3
Deut. 24:18De 5:15; 15:15; 16:12
Deut. 24:19Le 19:9
Deut. 24:19Le 23:22; Ru 2:16; Sl 41:1
Deut. 24:19De 15:10; Miy 11:24; 14:21; 19:17; Lu 6:38; 2Ak 9:6; 1Yo 3:17
Deut. 24:20Le 19:10; De 26:13
Deut. 24:22Eks 13:3
Deut. 24:222Ak 8:8
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 24:1-22

Deuteronomo

24 “Mwamuna akatenga mkazi kuti akhale mkazi wake, ndiyeno ngati mkaziyo sanamusangalatse chifukwa wam’peza ndi vuto linalake,+ azimulembera kalata yothetsera ukwati+ ndi kum’patsa m’manja mwake, n’kumuchotsa panyumba pake.+ 2 Pamenepo mkaziyo azituluka m’nyumba ya mwamunayo ndi kukakhala mkazi wa mwamuna wina.+ 3 Mwamuna wachiwiriyu akadana nayenso mkaziyo ndipo wamulembera kalata yothetsera ukwati n’kuiika m’manja mwake ndi kum’chotsa panyumba pake, kapena ngati mwamuna wachiwiriyu amene anam’tenga kukhala mkazi wake wamwalira, 4 mwamuna woyamba amene anam’chotsa uja sadzaloledwa kum’tenganso kuti akhale mkazi wake pambuyo poti waipitsidwa.+ Kuchita zimenezo n’konyansa pamaso pa Yehova, chotero usachimwitse dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa monga cholowa.

5 “Mwamuna akatenga mkazi watsopano,+ sayenera kukhala m’gulu lankhondo, ndiponso asakakamizidwe kuchita china chilichonse. Akhale kunyumba osachita zinthu zimenezi kwa chaka chimodzi kuti asangalatse mkazi amene watenga.+

6 “Munthu asalande mnzake mphero kapena mwala woperera monga chikole.+ Kumulanda zimenezi monga chikole ndiko kumulanda moyo.

7 “Munthu akaba+ mmodzi mwa abale ake, ana a Isiraeli, n’kumuchitira nkhanza ndiponso kum’gulitsa,+ wakuba munthuyo afe ndithu. Muzichotsa woipayo pakati panu.+

8 “Samalani ndi mliri wa khate+ ndi kuonetsetsa kuti mukuchita zonse zimene ansembe achilevi adzakulangizani.+ Muzichita mosamala zonse zimene ndawalamula.+ 9 Muzikumbukira zimene Yehova Mulungu wanu anachitira Miriamu panjira mutatuluka m’dziko la Iguputo.+

10 “Ukakongoza mnzako ngongole ya mtundu wina uliwonse,+ usamalowe m’nyumba yake kukatenga chimene walonjeza kukupatsa monga chikole.+ 11 Uziima panja, ndipo munthu amene wam’kongozayo azibweretsa yekha chikolecho kwa iwe, panjapo. 12 Ngati munthuyo ndi wovutika, usagone ndi chinthu chake chimene wakupatsa monga chikolecho.+ 13 Uzionetsetsa kuti wam’bwezera chikolecho dzuwa likangolowa,+ kuti akagone m’chovala chake.+ Pamenepo adzakudalitsa,+ ndipo udzakhala utachita chilungamo pamaso pa Yehova Mulungu wako.+

14 “Usachitire chinyengo waganyu wovutika ndiponso wosauka n’kumubera, kaya akhale mmodzi wa abale ako kapena mmodzi mwa alendo okhala m’dziko lanu, amene ali m’mizinda yanu.+ 15 Uzim’patsa malipiro ake+ tsiku lililonse, ndipo dzuwa lisalowe usanam’patse malipiro ake chifukwa iye ndi wovutika. Iye akuyembekezera malipiro akewo mwachidwi, ndipo angafuule kwa Yehova chifukwa cha zimene iweyo wam’chitira,+ iwe n’kupezeka kuti wachimwa.+

16 “Abambo asaphedwe chifukwa cha machimo a ana, ndipo ana asaphedwe chifukwa cha machimo a abambo.+ Aliyense aziphedwa chifukwa cha tchimo lake.+

17 “Usapotoze chiweruzo cha mlandu wa mlendo+ kapena mlandu wa mwana wamasiye,*+ ndipo usalande mkazi wamasiye chovala chake monga chikole.+ 18 Uzikumbukira kuti unali kapolo m’dziko la Iguputo, ndipo Yehova Mulungu wako anakuwombola kumeneko.+ N’chifukwa chake ndikukulamula kuti uzichita zimenezi.

19 “Ukaiwala mtolo wa tirigu pokolola m’munda wako,+ usabwerere kukatenga mtolowo. Uzisiyira mlendo wokhala m’dziko lanu, mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye.+ Uzichita zimenezi kuti Yehova Mulungu wako akudalitse pa chilichonse chimene dzanja lako likuchita.+

20 “Pokolola maolivi mwa kukwapula mitengo yake, usabwerere m’mbuyo kukaona ngati m’nthambi zake muli zipatso zotsala. Zimenezo zikhale za mlendo wokhala m’dziko lanu, mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye.+

21 “Pokolola mphesa m’munda wako, usabwerere kukakunkha zotsala. Mphesa zotsalazo zikhale za mlendo wokhala m’dziko lanu, mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye. 22 Uzikumbukira kuti unali kapolo m’dziko la Iguputo.+ N’chifukwa chake ndikukulamula kuti uzichita zimenezi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena