Genesis 39:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Koma Yosefe anali kukana+ ndi kuuza mkazi wa mbuye wakeyo kuti: “Chifukwa cha ine, mbuye wanga sadera nkhawa za chilichonse m’nyumba muno, ndipo chilichonse chimene iye ali nacho wachipereka m’manja mwanga.+ Salimo 105:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Mawu a Yehova anamuyenga,+Kufikira pamene lonjezo la Mulungu linakwaniritsidwa.+ Salimo 119:86 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 86 Malamulo anu onse ndi odalirika.+Odzikuza andizunza popanda chifukwa. Chonde, ndithandizeni.+ Danieli 6:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Mulungu wanga+ watumiza mngelo wake+ kudzatseka pakamwa pa mikango.+ Chotero mikangoyo sinandivulaze, chifukwa iye sanandipeze ndi mlandu uliwonse+ ndiponso sindinakulakwireni chilichonse inu mfumu.”+ Yohane 15:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Zili choncho kuti mawu olembedwa m’Chilamulo akwaniritsidwe. Mawu ake ndi akuti, ‘Anadana nane popanda chifukwa.’+ Aheberi 12:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Zoonadi, palibe chilango chimene chimamveka chosangalatsa pa nthawi yomwe ukuchilandira, koma chimakhala chowawa.+ Komabe pambuyo pake, kwa anthu amene aphunzirapo kanthu pa chilangocho, chimabala chipatso chamtendere,+ chomwe ndi chilungamo.+ 1 Petulo 3:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Pakuti ndi bwino kuvutika chifukwa chochita zabwino,+ ngati Mulungu walola, kusiyana ndi kuvutika chifukwa chochita zoipa.+
8 Koma Yosefe anali kukana+ ndi kuuza mkazi wa mbuye wakeyo kuti: “Chifukwa cha ine, mbuye wanga sadera nkhawa za chilichonse m’nyumba muno, ndipo chilichonse chimene iye ali nacho wachipereka m’manja mwanga.+
22 Mulungu wanga+ watumiza mngelo wake+ kudzatseka pakamwa pa mikango.+ Chotero mikangoyo sinandivulaze, chifukwa iye sanandipeze ndi mlandu uliwonse+ ndiponso sindinakulakwireni chilichonse inu mfumu.”+
25 Zili choncho kuti mawu olembedwa m’Chilamulo akwaniritsidwe. Mawu ake ndi akuti, ‘Anadana nane popanda chifukwa.’+
11 Zoonadi, palibe chilango chimene chimamveka chosangalatsa pa nthawi yomwe ukuchilandira, koma chimakhala chowawa.+ Komabe pambuyo pake, kwa anthu amene aphunzirapo kanthu pa chilangocho, chimabala chipatso chamtendere,+ chomwe ndi chilungamo.+
17 Pakuti ndi bwino kuvutika chifukwa chochita zabwino,+ ngati Mulungu walola, kusiyana ndi kuvutika chifukwa chochita zoipa.+