-
Salimo 135:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Amene anachita zimenezi ndi amene anakantha mitundu yambiri+
Ndi kupha mafumu amphamvu.+
-
Salimo 136:19Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
19 Iye anapha Sihoni mfumu ya Aamori:+
Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+
-
-
-