Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 26:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kuwonjezera apo, ku Yerusalemu anapanga makina ankhondo opangidwa ndi anthu aluso, oti aziwaika pansanja+ ndi pamakona a mpanda, kuti aziponyera mivi ndi miyala ikuluikulu. Chotero anatchuka+ mpaka kutali kwambiri, popeza anathandizidwa kwambiri mpaka anakhala wamphamvu.

  • Mlaliki 9:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Panali mzinda winawake waung’ono ndipo mumzindamo munali amuna ochepa. Kenako kunabwera mfumu yamphamvu ndipo inazungulira mzindawo, n’kuunjika milu ikuluikulu yadothi yoti imenyerepo nkhondo.+

  • Yesaya 37:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 “‘Chotero Yehova wanena izi zokhudza mfumu ya Asuri:+ “Sadzalowa mumzinda uno,+ kapena kuponyamo muvi, kapena kufikamo ndi chishango, kapenanso kumanga chiunda chomenyerapo nkhondo pafupi ndi mpanda wa mzindawu atauzungulira.”’+

  • Yeremiya 6:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Pakuti Yehova wa makamu wanena kuti: “Dulani mitengo+ kuti tipangire Yerusalemu chiunda chomenyerapo nkhondo.*+ Yerusalemu ndi mzinda woyenera kuimbidwa mlandu.+ Mkati mwake muli kuponderezana kokhakokha.+

  • Ezekieli 17:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Farao sadzamutumizira gulu lalikulu la asilikali ndi khamu la anthu kuti amuthandize pankhondo.+ Sadzamuthandiza mwa kumanga chiunda chomenyerapo nkhondo ndiponso mpanda womenyerapo nkhondo n’cholinga chakuti aphe anthu ambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena