Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 34:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Anamuonetsa Negebu+ ndi Chigawo*+ cha Yorodano, chigwa cha ku Yeriko, mzinda wa mitengo ya kanjedza,+ mpaka ku Zowari.+

  • Oweruza 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndiyeno ana a munthu wa mtundu wachikeni,+ amene anali apongozi ake a Mose,+ anatuluka mumzinda wa mitengo ya kanjedza+ pamodzi ndi ana a Yuda kukalowa m’chipululu cha Yuda, chimene chili kum’mwera kwa Aradi.+ Motero iwo anayamba kukhala pamodzi ndi anthuwo.+

  • 2 Mbiri 28:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako amuna amene anachita kusankhidwa powatchula mayina+ ananyamuka n’kutenga anthu ogwidwawo. Anthu onse amene sanavale* zovala anawaveka zovala+ zimene anafunkha ndipo anawavekanso nsapato. Anawapatsa chakudya+ ndi zakumwa,+ ndipo anawadzoza mafuta. Kuwonjezera apo, aliyense amene anali kuyenda movutikira anamukweza+ pabulu. Atatero anatenga anthuwo n’kupita nawo ku Yeriko,+ kumzinda wa mitengo ya kanjedza,+ kufupi ndi abale awo. Pambuyo pake iwo anabwerera ku Samariya.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena