Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Usapereke umboni wonamizira mnzako.+

  • Salimo 52:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Lilime lako limakonza chiwembu, ndipo ndi lakuthwa ngati lezala,+

      Limachita zachinyengo.+

  • Salimo 52:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Umakonda kwambiri zinthu zoipa kuposa zabwino,+

      Umakonda kwambiri kulankhula chinyengo kuposa kulankhula chilungamo.+ [Seʹlah.]

  • Miyambo 19:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mboni yonama sidzalephera kulangidwa,+ ndipo wolankhula mabodza sadzapulumuka.+

  • Miyambo 25:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Munthu wonenera mnzake umboni wonama ali ngati chibonga cha kunkhondo, lupanga, ndi muvi wakuthwa.+

  • Miyambo 29:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mtsogoleri akamamvera mabodza, onse omutumikira adzakhala oipa.+

  • Ezekieli 22:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mwa iwe muli anthu amiseche amene akukhetsa magazi.+ Iwo amadya chakudya choperekedwa nsembe kwa mafano m’mapiri.+ Achita khalidwe lotayirira mwa iwe.+

  • Mateyu 26:59
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 59 Pa nthawiyi ansembe aakulu ndi Khoti lonse Lalikulu la Ayuda* anali kufunafuna umboni wonama kuti amunamizire mlandu Yesu ndi kumupha+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena