Oweruza 20:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Choncho ndinatenga mdzakazi wanga ndi kum’duladula, n’kutumiza ziwalozo m’dera lililonse la cholowa cha Isiraeli.+ Ndinatero chifukwa iwo anachita khalidwe lotayirira+ komanso chinthu chopusa ndi chochititsa manyazi mu Isiraeli.+ Salimo 26:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 M’manja mwa anthu amenewa muli khalidwe lotayirira,+Ndipo m’dzanja lawo lamanja mwadzaza ziphuphu.+ Miyambo 10:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Kwa wopusa, kusonyeza khalidwe lotayirira kuli ngati masewera,+ koma nzeru zimakhala ndi munthu wozindikira.+ Yeremiya 13:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Chigololo chako,+ kumemesa* kwako,+ khalidwe lako lotayirira la uhule, zonsezi zidzaonekera. Ndaona zinthu zako zonyansa pamapiri kuthengo.+ Tsoka kwa iwe Yerusalemu! Sungakhale woyera.+ Kodi udzakhalabe wosayera kufikira liti?”+ Ezekieli 16:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Tsopano ine ndidzakutambasulira dzanja langa+ ndipo ndidzakuchepetsera gawo lako.+ Ndidzakupereka ku zilakolako+ za akazi odana nawe,+ ana aakazi a Afilisiti,+ akazi amene akuchita manyazi ndi khalidwe lako lotayirira.+ 2 Petulo 2:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Koma anapulumutsa Loti, munthu wolungama+ amene anavutika mtima kwambiri ndi kulowerera kwa anthu ophwanya malamulo mu khalidwe lawo lotayirira.+
6 Choncho ndinatenga mdzakazi wanga ndi kum’duladula, n’kutumiza ziwalozo m’dera lililonse la cholowa cha Isiraeli.+ Ndinatero chifukwa iwo anachita khalidwe lotayirira+ komanso chinthu chopusa ndi chochititsa manyazi mu Isiraeli.+
10 M’manja mwa anthu amenewa muli khalidwe lotayirira,+Ndipo m’dzanja lawo lamanja mwadzaza ziphuphu.+
23 Kwa wopusa, kusonyeza khalidwe lotayirira kuli ngati masewera,+ koma nzeru zimakhala ndi munthu wozindikira.+
27 Chigololo chako,+ kumemesa* kwako,+ khalidwe lako lotayirira la uhule, zonsezi zidzaonekera. Ndaona zinthu zako zonyansa pamapiri kuthengo.+ Tsoka kwa iwe Yerusalemu! Sungakhale woyera.+ Kodi udzakhalabe wosayera kufikira liti?”+
27 Tsopano ine ndidzakutambasulira dzanja langa+ ndipo ndidzakuchepetsera gawo lako.+ Ndidzakupereka ku zilakolako+ za akazi odana nawe,+ ana aakazi a Afilisiti,+ akazi amene akuchita manyazi ndi khalidwe lako lotayirira.+
7 Koma anapulumutsa Loti, munthu wolungama+ amene anavutika mtima kwambiri ndi kulowerera kwa anthu ophwanya malamulo mu khalidwe lawo lotayirira.+