Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 13:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Dziko limene latsala ndi ili:+ Madera onse a Afilisiti+ ndi madera onse a Agesuri.+

  • Oweruza 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pali mitundu+ imene Yehova anailola kukhalabe m’dzikoli n’cholinga choti ayese+ nayo Aisiraeli, kutanthauza Aisiraeli onse amene sanaonepo iliyonse mwa nkhondo zimene mtunduwo unamenya m’dziko la Kanani.+

  • Oweruza 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mitunduyo ndi olamulira asanu ogwirizana+ a Afilisiti,+ Akanani onse,+ ngakhalenso Asidoni+ ndi Ahivi+ okhala m’phiri la Lebanoni,+ kuchokera kuphiri la Baala-herimoni+ mpaka kumalire a dera la Hamati.+

  • 1 Samueli 9:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Mawa nthawi ngati ino ndikutumizira munthu kuchokera kudera la Benjamini,+ ndipo udzam’dzoze+ kukhala mtsogoleri wa anthu anga Aisiraeli. Iye adzapulumutsa anthu anga m’manja mwa Afilisiti,+ chifukwa ndaona kusautsika kwawo ndipo ndamva kulira kwawo.”+

  • 1 Samueli 14:52
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 52 M’masiku onse a Sauli, Afilisiti anali kupanikizidwa ndi nkhondo.+ Ndipo Sauli akaona munthu aliyense wamphamvu kapena wolimba mtima, anali kum’tenga kuti akhale msilikali wake.+

  • Amosi 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Yehova akufunsa kuti, ‘Inu ana a Isiraeli, kodi simuli ngati ana a Akusi kwa ine? Kodi si ndine amene ndinatulutsa Aisiraeli m’dziko la Iguputo,+ amenenso ndinatulutsa Afilisiti+ ku Kerete komanso Asiriya ku Kiri?’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena