-
1 Samueli 16:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Patapita nthawi, Yehova anauza Samueli kuti: “Kodi ulirira Sauli+ mpaka liti, pamene ine ndamukana kuti alamulire monga mfumu ya Isiraeli?+ Thira mafuta m’nyanga yako+ ndipo unyamuke. Ndikutumiza kwa Jese+ wa ku Betelehemu, chifukwa ndapeza munthu pakati pa ana ake aamuna woti akhale mfumu yanga.”+
-
-
Mateyu 1:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Jese anabereka mfumu+ Davide.+
Davide anabereka Solomo,+ yemwe mayi ake anali mkazi wa Uriya.
-
Luka 3:32Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
mwana wa Obedi,+
mwana wa Boazi,+
mwana wa Salimoni,+
mwana wa Naasoni,+
-
-
-