Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 8:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Benaya+ mwana wa Yehoyada anali mtsogoleri wa Akereti+ ndi Apeleti.+ Ana aamuna a Davide anakhala ansembe.*+

  • 2 Samueli 20:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Choncho asilikali a Yowabu,+ Akereti,+ Apeleti+ ndi amuna onse amphamvu anayamba kumuthamangitsa. Iwo anatuluka mu Yerusalemu ndi kuthamangitsa Sheba mwana wa Bikiri.

  • 1 Mafumu 1:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Wansembe Zadoki,+ mneneri Natani,+ Benaya+ mwana wa Yehoyada, Akereti+ ndi Apeleti+ anatsetsereka n’kukakweza Solomo panyulu yaikazi ya Mfumu Davide,+ kenako anapita naye ku Gihoni.+

  • 1 Mbiri 18:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Benaya+ mwana wa Yehoyada+ anali mtsogoleri wa Akereti+ ndi Apeleti,+ ndipo ana aamuna a Davide ndiwo anali ndi udindo waukulu kwambiri pamaso pa mfumu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena