Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano Adoni-zedeki, mfumu ya Yerusalemu anamva zakuti Yoswa walanda mzinda wa Ai+ ndi kuuwononga.+ Iye anamva kuti Yoswa wawononga mzindawo ndi kupha mfumu yake+ monga anachitira ndi mzinda wa Yeriko+ ndi mfumu yake.+ Anamvanso kuti anthu okhala ku Gibeoni apangana za mtendere ndi Aisiraeli+ ndipo akukhala pakati pawo. Atangomva zimenezi,

  • Yoswa 10:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa tsiku limene Yehova anapereka Aamori kwa ana a Isiraeli, Yoswa analankhula ndi Yehova pamaso pa Aisiraeli kuti:

      “Dzuwa iwe,+ ima pamwamba pa Gibeoni,+

      Ndipo iwe mwezi, ima pamwamba pa chigwa cha Aijaloni.”+

  • Yoswa 18:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Kunalinso Gibeoni,+ Rama, Beeroti,

  • Yoswa 21:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kuchokera m’fuko la Benjamini, anawapatsa Gibeoni+ ndi malo ake odyetserako ziweto, Geba+ ndi malo ake odyetserako ziweto,

  • 2 Samueli 20:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pamene anali pafupi ndi mwala waukulu umene uli ku Gibeoni,+ Amasa+ anabwera kudzakumana nawo. Tsopano Yowabu anali atavala malaya ankhondo ndi lamba. Iye anali ataika lupanga m’chimake ndi kulipachika m’chiuno mwake. Atayandikira Amasa, lupangalo linagwa pansi.

  • 1 Mafumu 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ku Gibeoniko, Yehova Mulungu anaonekera+ kwa Solomo m’maloto+ usiku ndipo anati: “Pempha chimene ukufuna kuti ndikupatse.”+

  • 1 Mbiri 14:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Choncho Davide anachitadi monga mmene Mulungu woona anamulamulira,+ moti iwo anapha asilikali a Afilisiti kuchokera ku Gibeoni+ mpaka kukafika ku Gezeri.+

  • 2 Mbiri 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Kenako Solomo ndi mpingo wonsewo anapitira limodzi kumalo okwezeka a ku Gibeoni.+ Anapita kumeneko chifukwa ndi kumene kunali chihema chokumanako+ cha Mulungu woona, chimene Mose mtumiki+ wa Yehova anapanga m’chipululu.

  • Yesaya 28:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Yehova adzaimirira monga mmene anachitira paphiri la Perazimu.+ Adzakalipa ngati mmene anachitira m’chigwa cha kufupi ndi Gibeoni+ kuti achite ntchito yake. Ntchito yakeyo ndi yodabwitsa. Adzakalipa kuti achite zochita zake. Zochita zakezo n’zachilendo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena