Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 14:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pamenepo Mose anauza anthuwo kuti: “Musachite mantha.+ Chilimikani ndi kuona chipulumutso cha Yehova chimene akuchitireni lero.+ Pakuti Aiguputo amene mukuwaona lerowa simudzawaonanso, ndithu, simudzawaonanso.+

  • Ekisodo 15:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mphamvu ndi nyonga yanga ndi Ya,*+ pakuti wandipulumutsa.+

      Ameneyu ndi Mulungu wanga, ndidzam’tamanda.+ Ndiye Mulungu wa atate anga,+ ndidzam’kweza.+

  • 1 Samueli 2:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ndiyeno Hana anayamba kupemphera+ kuti:

      “Mtima wanga ukukondwera mwa Yehova,+

      Nyanga* yanga yakwezekadi kudzera mwa Yehova.+

      Ndikutsutsana ndi adani anga molimba mtima,

      Pakuti ndikukondwera ndi chipulumutso chochokera kwa inu.+

  • 1 Samueli 11:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Koma Sauli anayankha kuti: “Lero pasaphedwe munthu aliyense,+ chifukwa Yehova watipulumutsa mu Isiraeli.”+

  • 1 Mbiri 16:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Imbirani Yehova, inu nonse okhala padziko lapansi!+

      Tsiku ndi tsiku lengezani chipulumutso chimene amapereka!+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena