Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 33:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Palibe wina wofanana ndi Mulungu woona+ wa Yesuruni,+

      Amene amayenda m’mlengalenga pokuthandiza,+

      Amene amayenda pamitambo mu ulemerero wake.+

  • Salimo 18:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iye anafika atakwera pakerubi wouluka.+

      Mulungu anali kuuluka mwaliwiro pamapiko a cholengedwa chauzimu.*+

  • Salimo 104:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu munamanga zipinda za m’mwamba pamadzi pogwiritsa ntchito mitanda,+

      Munapanga mitambo kukhala galeta lanu,+

      Mumayenda pamapiko a mphepo.+

  • Yesaya 19:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Uwu ndi uthenga wokhudza Iguputo:+ Taonani! Yehova wakwera mtambo wothamanga+ ndipo akubwera mu Iguputo. Milungu yopanda pake ya ku Iguputo idzanjenjemera chifukwa chomuopa+ ndipo mitima ya Aiguputo idzasungunuka mkati mwa dzikolo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena