Genesis 18:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Potsirizira pake anati: “Chonde Yehova, pepani, musandipsere mtima,+ tandilolani ndilankhule komaliza kokhaka.+ Nanga mutapezeka 10?” Iye anayankha kuti: “Sindiwononga mzindawo chifukwa cha 10 amenewo.”+ Salimo 12:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Ndipulumutseni,+ inu Yehova, pakuti anthu okhulupirika atha.+Anthu okhulupirika atheratu pakati pa ana a anthu. Salimo 14:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Onse apatuka,+ ndipo onsewo ndi achinyengo.+Palibe aliyense amene akuchita zabwino,+Palibiretu ndi mmodzi yemwe.+ Ezekieli 22:29 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 29 Anthu a m’dzikolo abera anthu pochita zachinyengo+ ndiponso zauchifwamba.+ Iwo akuzunza anthu osautsika ndi osauka.+ Abera mlendo pochita zachinyengo komanso zopanda chilungamo.’+ Amosi 5:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Mukuweruza mopanda chilungamo,+ choncho moyo wakhala wowawa ndi wosautsa kwa anthu, pakuti inuyo mwakana chilungamo.+ Mika 7:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Anthu okhulupirika atha padziko lapansi, ndipo pakati pa anthu palibe munthu wowongoka mtima.+ Onse amadikirira anzawo kuti akhetse magazi.+ Aliyense amasaka m’bale wake ndi ukonde.+
32 Potsirizira pake anati: “Chonde Yehova, pepani, musandipsere mtima,+ tandilolani ndilankhule komaliza kokhaka.+ Nanga mutapezeka 10?” Iye anayankha kuti: “Sindiwononga mzindawo chifukwa cha 10 amenewo.”+
12 Ndipulumutseni,+ inu Yehova, pakuti anthu okhulupirika atha.+Anthu okhulupirika atheratu pakati pa ana a anthu.
3 Onse apatuka,+ ndipo onsewo ndi achinyengo.+Palibe aliyense amene akuchita zabwino,+Palibiretu ndi mmodzi yemwe.+
29 Anthu a m’dzikolo abera anthu pochita zachinyengo+ ndiponso zauchifwamba.+ Iwo akuzunza anthu osautsika ndi osauka.+ Abera mlendo pochita zachinyengo komanso zopanda chilungamo.’+
7 Mukuweruza mopanda chilungamo,+ choncho moyo wakhala wowawa ndi wosautsa kwa anthu, pakuti inuyo mwakana chilungamo.+
2 Anthu okhulupirika atha padziko lapansi, ndipo pakati pa anthu palibe munthu wowongoka mtima.+ Onse amadikirira anzawo kuti akhetse magazi.+ Aliyense amasaka m’bale wake ndi ukonde.+