Salimo 74:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Iwo atentha malo anu opatulika.+Aipitsa ndi kugwetsera pansi chihema chokhala ndi dzina lanu.+ Salimo 79:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 79 Inu Mulungu, anthu a mitundu ina alowa m’dziko limene ndilo cholowa chanu.+Aipitsa kachisi wanu woyera.+Awononga Yerusalemu ndi kumusandutsa bwinja.+ Yeremiya 7:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 ndidzachita zofanana ndi zimene ndinachita ku Silo.+ Ndidzachita zimenezi panyumba imene ikutchedwa ndi dzina langa,+ imene inu mukuidalira,+ ndiponso malo amene ndinapatsa inu ndi makolo anu. Maliro 1:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Mdani watambasula dzanja lake n’kutenga zinthu+ zake zonse zabwino.Yerusalemu waona mitundu ina itabwera ndi kulowa m’malo ake opatulika,+Mitundu imene munalamula kuti isalowe mumpingo wanu. Maliro 2:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Yehova wataya guwa lake lansembe.+ Iye wanyoza malo ake opatulika.+Wapereka m’manja mwa adani makoma* a nsanja zake zokhalamo.+Iwo afuula m’nyumba ya Yehova ngati pa tsiku lachikondwerero.+ Ezekieli 9:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Iye anawauzanso kuti: “Ipitsani nyumbayi ndipo mudzaze mabwalo ake ndi mitembo ya anthu ophedwa.+ Pitani!” Iwo anapitadi n’kukapha anthu mumzindamo.
79 Inu Mulungu, anthu a mitundu ina alowa m’dziko limene ndilo cholowa chanu.+Aipitsa kachisi wanu woyera.+Awononga Yerusalemu ndi kumusandutsa bwinja.+
14 ndidzachita zofanana ndi zimene ndinachita ku Silo.+ Ndidzachita zimenezi panyumba imene ikutchedwa ndi dzina langa,+ imene inu mukuidalira,+ ndiponso malo amene ndinapatsa inu ndi makolo anu.
10 Mdani watambasula dzanja lake n’kutenga zinthu+ zake zonse zabwino.Yerusalemu waona mitundu ina itabwera ndi kulowa m’malo ake opatulika,+Mitundu imene munalamula kuti isalowe mumpingo wanu.
7 Yehova wataya guwa lake lansembe.+ Iye wanyoza malo ake opatulika.+Wapereka m’manja mwa adani makoma* a nsanja zake zokhalamo.+Iwo afuula m’nyumba ya Yehova ngati pa tsiku lachikondwerero.+
7 Iye anawauzanso kuti: “Ipitsani nyumbayi ndipo mudzaze mabwalo ake ndi mitembo ya anthu ophedwa.+ Pitani!” Iwo anapitadi n’kukapha anthu mumzindamo.