Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 74:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iwo atentha malo anu opatulika.+

      Aipitsa ndi kugwetsera pansi chihema chokhala ndi dzina lanu.+

  • Salimo 79:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 79 Inu Mulungu, anthu a mitundu ina alowa m’dziko limene ndilo cholowa chanu.+

      Aipitsa kachisi wanu woyera.+

      Awononga Yerusalemu ndi kumusandutsa bwinja.+

  • Yeremiya 7:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 ndidzachita zofanana ndi zimene ndinachita ku Silo.+ Ndidzachita zimenezi panyumba imene ikutchedwa ndi dzina langa,+ imene inu mukuidalira,+ ndiponso malo amene ndinapatsa inu ndi makolo anu.

  • Maliro 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mdani watambasula dzanja lake n’kutenga zinthu+ zake zonse zabwino.

      Yerusalemu waona mitundu ina itabwera ndi kulowa m’malo ake opatulika,+

      Mitundu imene munalamula kuti isalowe mumpingo wanu.

  • Maliro 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Yehova wataya guwa lake lansembe.+ Iye wanyoza malo ake opatulika.+

      Wapereka m’manja mwa adani makoma* a nsanja zake zokhalamo.+

      Iwo afuula m’nyumba ya Yehova ngati pa tsiku lachikondwerero.+

  • Ezekieli 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Iye anawauzanso kuti: “Ipitsani nyumbayi ndipo mudzaze mabwalo ake ndi mitembo ya anthu ophedwa.+ Pitani!” Iwo anapitadi n’kukapha anthu mumzindamo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena