Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Akorinto 16
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

1 Akorinto 16:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 24:17; Aro 15:26
  • +2Ak 8:4
  • +Aga 1:2

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    11/1/1998, tsa. 24

1 Akorinto 16:2

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu,

    11/2023, tsa. 3

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 55

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/2013, tsa. 14

    7/15/2008, tsa. 27

    12/1/2002, tsa. 5

    11/1/2002, ptsa. 26-30

    11/1/1998, tsa. 24

    12/1/1994, tsa. 17

    1/15/1992, tsa. 17

    4/15/1991, tsa. 27

    12/1/1989, tsa. 24

    Utumiki wa Ufumu,

    1/2002, tsa. 2

1 Akorinto 16:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ak 8:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    7/15/1998, tsa. 7

    12/1/1989, tsa. 24

1 Akorinto 16:4

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    7/15/1998, tsa. 7

    12/1/1989, tsa. 24

1 Akorinto 16:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 19:21; 2Ak 1:16

1 Akorinto 16:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 17:15; Aro 15:24; 3Yo 6

1 Akorinto 16:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 20:2
  • +Yak 4:15; 1Yo 5:14
  • +Mac 18:21

1 Akorinto 16:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 19:1

1 Akorinto 16:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 19:10

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/2008, ptsa. 18-19

    12/15/1990, tsa. 23

1 Akorinto 16:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 16:1; Afi 2:19
  • +Afi 2:20; 1Ti 4:14

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    5/15/2009, ptsa. 14-15

1 Akorinto 16:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ti 4:12

1 Akorinto 16:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 18:24

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/1996, tsa. 22

1 Akorinto 16:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1At 5:6
  • +1Ak 15:58; Afi 1:27
  • +Mac 4:29
  • +Aef 6:10; Akl 1:11

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    9/15/2015, ptsa. 13-17

    1/1/2003, ptsa. 18-19

    4/1/2002, ptsa. 15, 27-28

    4/15/1990, ptsa. 26-28

    Galamukani!,

    5/8/2000, tsa. 30

    Utumiki wa Ufumu,

    2/2000, tsa. 8

1 Akorinto 16:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ak 13:4; 1Pe 4:8

1 Akorinto 16:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 16:5
  • +2Ak 8:4; Ahe 6:10

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/1988, ptsa. 19-20

1 Akorinto 16:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Afi 2:29; 1At 5:12; 1Ti 5:17

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/1988, ptsa. 19-20

1 Akorinto 16:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ak 1:16

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/1988, ptsa. 19-20

1 Akorinto 16:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Ak 7:13
  • +Afi 2:29

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/1/1988, ptsa. 19-20

1 Akorinto 16:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 16:5
  • +Fili 2

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    8/15/2007, tsa. 10

1 Akorinto 16:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 16:16

1 Akorinto 16:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2At 3:17; Fili 19

1 Akorinto 16:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aga 1:8
  • +Chv 22:20

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

1 Akor. 16:1Mac 24:17; Aro 15:26
1 Akor. 16:12Ak 8:4
1 Akor. 16:1Aga 1:2
1 Akor. 16:32Ak 8:19
1 Akor. 16:5Mac 19:21; 2Ak 1:16
1 Akor. 16:6Mac 17:15; Aro 15:24; 3Yo 6
1 Akor. 16:7Mac 20:2
1 Akor. 16:7Yak 4:15; 1Yo 5:14
1 Akor. 16:7Mac 18:21
1 Akor. 16:8Mac 19:1
1 Akor. 16:9Mac 19:10
1 Akor. 16:10Mac 16:1; Afi 2:19
1 Akor. 16:10Afi 2:20; 1Ti 4:14
1 Akor. 16:111Ti 4:12
1 Akor. 16:12Mac 18:24
1 Akor. 16:131At 5:6
1 Akor. 16:131Ak 15:58; Afi 1:27
1 Akor. 16:13Mac 4:29
1 Akor. 16:13Aef 6:10; Akl 1:11
1 Akor. 16:141Ak 13:4; 1Pe 4:8
1 Akor. 16:15Aro 16:5
1 Akor. 16:152Ak 8:4; Ahe 6:10
1 Akor. 16:16Afi 2:29; 1At 5:12; 1Ti 5:17
1 Akor. 16:171Ak 1:16
1 Akor. 16:182Ak 7:13
1 Akor. 16:18Afi 2:29
1 Akor. 16:19Aro 16:5
1 Akor. 16:19Fili 2
1 Akor. 16:20Aro 16:16
1 Akor. 16:212At 3:17; Fili 19
1 Akor. 16:22Aga 1:8
1 Akor. 16:22Chv 22:20
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
1 Akorinto 16:1-24

1 Akorinto

16 Tsopano ponena za chopereka+ chopita kwa oyerawo,+ inunso tsatirani malangizo amene ndinapereka ku mipingo ya ku Galatiya.+ 2 Tsiku lililonse loyamba la mlungu, aliyense wa inu aziika kenakake pambali kunyumba kwake malinga ndi mmene zinthu zikuyendera pa moyo wake, kuti ndikadzafika, zopereka zisadzaperekedwe pa nthawi imeneyo. 3 Koma ndikadzafika kumeneko, amuna alionse amene mungawavomereze m’makalata,+ ndidzawatuma kuti adzapititse mphatso yanu yachifundoyo ku Yerusalemu. 4 Komabe, ngati kudzakhala kofunika kuti inenso ndidzapite, tidzapitira limodzi.

5 Ndidzafika kwa inu pochokera ku Makedoniya, pakuti ndipita ku Makedoniya.+ 6 Mwina ndidzakhala nanu pang’ono kumeneko, ngakhalenso kwa nyengo yonse yachisanu, kuti mudzandiperekeze+ kumene ndizidzapitako. 7 Pakuti sindikufuna kukuonani panopo mongodutsa chabe, koma ndikufuna kuti ndidzakhale nanu kanthawi ndithu,+ ngati Yehova+ alola.+ 8 Koma ndikhalabe kuno ku Efeso+ mpaka chikondwerero cha Pentekosite, 9 pakuti khomo lalikulu la mwayi wautumiki landitsegukira,+ koma pali otsutsa ambiri.

10 Komabe, Timoteyo+ akadzafika mudzaonetsetse kuti asadzakhale ndi mantha pakati panu, pakuti iye akuchita ntchito ya Yehova,+ mmenenso ine ndikuchitira. 11 Choncho pasadzapezeke munthu womuderera.+ Mudzamuperekeze mu mtendere kuti adzafike kwa ine kunoko, pakuti ineyo ndikumuyembekezera pamodzi ndi abale.

12 Tsopano kunena za m’bale wathu Apolo,+ ndinamuchonderera kwambiri kuti abwere kwanuko pamodzi ndi abale, koma iye sanafune kubwera pa nthawi ino. Adzabwera akadzapeza mpata.

13 Khalani maso,+ limbani m’chikhulupiriro,+ pitirizani kuchita chamuna,+ khalani amphamvu.+ 14 Zonse zimene mukuchita, muzichite mwachikondi.+

15 Tsopano ndikukulimbikitsani mokudandaulirani, abale, kuti: Mukudziwa kuti banja la Sitefana ndilo chipatso choyambirira+ mu Akaya ndi kuti anadzipereka kutumikira oyera.+ 16 Inunso pitirizani kudzipereka kwa anthu ngati amenewo, ndi kwa aliyense wogwirizana nafe pa ntchitoyi, ndiponso wogwira ntchito molimbika.+ 17 Koma ndikusangalala kuti Sitefana+ ndi Fotunato ndi Akayiko ali kuno ndi ine, pakuti alowa m’malo mwanu. 18 Pakuti atsitsimutsa mtima wanga+ ndi wanunso. Chotero, anthu otere muziwalemekeza.+

19 Mipingo ya ku Asia ikupereka moni.+ Akula ndi Purisika, pamodzi ndi mpingo umene umasonkhana m’nyumba mwawo,+ akupereka moni wochokera pansi pa mtima kwa inu nonse, mwa Ambuye. 20 Abale onse akukupatsani moni. Mupatsane moni ndi kupsompsonana kopatulika.+

21 Tsopano landirani moni wanga wolemba ndekha ndi dzanja langa, ineyo Paulo.+

22 Ngati wina aliyense sakonda Ambuye, atembereredwe.+ Inde, idzani Ambuye!+ 23 Kukoma mtima kwakukulu kwa Ambuye Yesu kukhale nanu. 24 Nonsenu landirani chikondi changa mwa Khristu Yesu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena