Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 27:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Ndiyeno upange bwalo+ la chihema chopatulika. Kumbali ya ku Negebu, chakum’mwera, bwalolo ulitchinge ndi mpanda wa nsalu za ulusi wopota wabwino kwambiri.+ Mpandawo ukhale mikono 100 m’litali mwake kumbali imodziyo.

  • Ekisodo 38:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndiyeno anapanga bwalo la chihema chopatulika.+ Kumbali ya ku Negebu, chakum’mwera, bwalolo analitchinga ndi mpanda wa nsalu za ulusi wopota wabwino kwambiri. Mpandawo unali mikono 100 kutalika kwake kumbali imodziyo.+

  • Ekisodo 40:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Atatero anatchinga mpanda+ kuzungulira bwalo la chihema chopatulika ndi guwa lansembe, ndipo anakoloweka nsalu yotchinga pachipata cha bwalolo.+

      Chotero Mose anamaliza ntchitoyo.

  • Ezekieli 42:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno munthu uja anandiuza kuti: “Zipinda zodyeramo za kumpoto ndi za kum’mwera zimene zili moyang’anizana ndi mpata waukulu+ ndi zopatulika. M’zipinda zimenezi, ansembe otumikira+ Yehova amadyeramo zinthu zopatulika koposa.+ Mmenemo amaikamo zinthu zopatulika koposa, nsembe yambewu, nsembe yamachimo ndi nsembe ya kupalamula, chifukwa malo amenewa ndi oyera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena