Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 “Ndikudziwa bwino kuti zili choncho.

      Koma kodi munthu angakhale bwanji wosalakwa pa mlandu wotsutsana ndi Mulungu?+

  • Yobu 10:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ngati ndachimwa ndipo inu mwaona zonsezo,+

      Ndiponso simunandikhululukire zolakwa zanga,+

  • Salimo 103:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pakuti iye akudziwa bwino mmene anatiumbira,+

      Amakumbukira kuti ndife fumbi.+

  • Salimo 143:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Musandiimbe mlandu ine mtumiki wanu,+

      Pakuti palibe aliyense wamoyo amene angakhale wolungama pamaso panu.+

  • Yesaya 55:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Munthu woipa asiye njira yake+ ndipo wopweteka anzake asiye maganizo ake.+ Iye abwerere kwa Yehova ndipo adzamuchitira chifundo.+ Abwerere kwa Mulungu wathu, pakuti amakhululuka ndi mtima wonse.+

  • Danieli 9:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mulungu wanga, tcherani khutu lanu kuti mumve.+ Tsegulani maso anu kuti muone kuwonongeka kwathu ndi kwa mzinda wotchedwa ndi dzina lanu.+ Ifeyo tikukuchondererani, osati chifukwa cha zochita zathu zolungama,+ koma chifukwa cha chifundo chanu chachikulu.+

  • Aroma 3:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Chotero pamaso pake palibe munthu amene adzayesedwe wolungama+ mwa ntchito za chilamulo,+ popeza chilamulo chimachititsa kuti tidziwe uchimo molondola.+

  • Tito 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Iye sanatero chifukwa cha ntchito+ zolungama zimene tinachita+ ayi. Koma malinga ndi chifundo+ chake, anatipulumutsa mwa kutisambitsa+ ndipo chifukwa chakuti tinasambitsidwa choncho, tinafika ku moyo+ watsopano. Komanso, anatipulumutsa potisandutsa atsopano mwa mzimu woyera.+

  • Yakobo 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Paja tonsefe timapunthwa nthawi zambiri.+ Ngati wina sapunthwa pa mawu,+ ameneyo ndi munthu wangwiro,+ ndipo akhoza kulamuliranso thupi lake lonse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena