Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mafumu a dziko lapansi aima pamalo awo,+

      Ndipo nduna zapamwamba zasonkhana pamodzi mogwirizana.+

      Atero kuti alimbane ndi Yehova+ komanso wodzozedwa wake.+

  • Salimo 16:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti simudzasiya moyo wanga m’Manda.+

      Simudzalola kuti wokhulupirika wanu aone dzenje.+

  • Salimo 27:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Musandipereke kwa adani anga.+

      Pakuti mboni zonama zandiukira,+

      Chimodzimodzinso munthu wachiwawa.+

  • Salimo 69:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti kudzipereka kwambiri panyumba yanu kwandidya,+

      Ndipo mnyozo wa anthu amene akukutonzani wagwa pa ine.+

  • Salimo 78:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndidzatsegula pakamwa panga ndi kunena mwambi.+

      Ndidzanena mawu ophiphiritsa akalekale,+

  • Salimo 118:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mwala umene omanga nyumba anaukana+

      Wakhala mwala wofunika kwambiri wapakona.+

  • Salimo 132:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova walumbira kwa Davide,+

      Ndithudi sadzabweza mawu ake akuti:+

      “Ndidzaika pampando wako wachifumu+

      Chipatso cha mimba yako.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena