Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 26
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 26:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 6:1; 18:9

Deuteronomo 26:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:19; Le 23:10; Nu 18:12; 2Mb 31:5; Ne 10:35; Miy 3:9
  • +De 12:5; 2Mb 6:6

Deuteronomo 26:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 18:28
  • +Ge 17:8; 26:3; Sl 105:11; Ahe 6:13

Deuteronomo 26:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 28:5; 31:41, 42; Ho 12:12
  • +Ge 46:3; Mac 7:15
  • +Ge 46:27; De 7:7
  • +Eks 1:7; De 10:22; Sl 105:24

Deuteronomo 26:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 1:11; De 4:20

Deuteronomo 26:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 3:9; Sl 116:1
  • +Sl 102:20; Yes 59:1; 1Yo 5:15
  • +Eks 4:31; Mac 7:34

Deuteronomo 26:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 13:3; De 6:21
  • +Eks 6:6; De 4:34
  • +Eks 15:16; Yer 32:21
  • +Eks 7:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    10/15/2015, ptsa. 4-5

Deuteronomo 26:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 3:8; De 8:8; Eze 20:6

Deuteronomo 26:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 26:2
  • +Sl 95:6

Deuteronomo 26:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 12:7; Sl 32:11; 63:5; 68:3; Afi 4:4
  • +De 16:14

Deuteronomo 26:12

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu ake enieni, “mwana wamwamuna wopanda bambo.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 12:6; 14:22
  • +De 14:28
  • +De 14:29; Miy 14:21; 1Yo 3:17

Deuteronomo 26:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yak 1:27
  • +Sl 119:141; Miy 3:1; Mac 24:16

Deuteronomo 26:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 102:19; Yes 40:22; 63:15
  • +Eks 23:25; Sl 28:9; 115:12
  • +De 8:8
  • +Ge 15:18; 26:3; Ahe 6:13

Deuteronomo 26:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:1; 6:1; 11:1
  • +De 6:6; Sl 78:7; 119:34; 1Yo 5:3
  • +De 13:3

Deuteronomo 26:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 10:11; 26:46; Sl 119:5
  • +De 13:18; Mla 12:13
  • +Le 19:37; Sl 19:9
  • +De 15:5

Deuteronomo 26:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:5; De 14:2; Sl 135:4
  • +De 29:13

Deuteronomo 26:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 4:8; 28:1; Sl 148:14
  • +De 7:6; 28:9

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 26:1De 6:1; 18:9
Deut. 26:2Eks 23:19; Le 23:10; Nu 18:12; 2Mb 31:5; Ne 10:35; Miy 3:9
Deut. 26:2De 12:5; 2Mb 6:6
Deut. 26:3Nu 18:28
Deut. 26:3Ge 17:8; 26:3; Sl 105:11; Ahe 6:13
Deut. 26:5Ge 28:5; 31:41, 42; Ho 12:12
Deut. 26:5Ge 46:3; Mac 7:15
Deut. 26:5Ge 46:27; De 7:7
Deut. 26:5Eks 1:7; De 10:22; Sl 105:24
Deut. 26:6Eks 1:11; De 4:20
Deut. 26:7Eks 3:9; Sl 116:1
Deut. 26:7Sl 102:20; Yes 59:1; 1Yo 5:15
Deut. 26:7Eks 4:31; Mac 7:34
Deut. 26:8Eks 13:3; De 6:21
Deut. 26:8Eks 6:6; De 4:34
Deut. 26:8Eks 15:16; Yer 32:21
Deut. 26:8Eks 7:3
Deut. 26:9Eks 3:8; De 8:8; Eze 20:6
Deut. 26:10De 26:2
Deut. 26:10Sl 95:6
Deut. 26:11De 12:7; Sl 32:11; 63:5; 68:3; Afi 4:4
Deut. 26:11De 16:14
Deut. 26:12De 12:6; 14:22
Deut. 26:12De 14:28
Deut. 26:12De 14:29; Miy 14:21; 1Yo 3:17
Deut. 26:13Yak 1:27
Deut. 26:13Sl 119:141; Miy 3:1; Mac 24:16
Deut. 26:15Sl 102:19; Yes 40:22; 63:15
Deut. 26:15Eks 23:25; Sl 28:9; 115:12
Deut. 26:15De 8:8
Deut. 26:15Ge 15:18; 26:3; Ahe 6:13
Deut. 26:16De 4:1; 6:1; 11:1
Deut. 26:16De 6:6; Sl 78:7; 119:34; 1Yo 5:3
Deut. 26:16De 13:3
Deut. 26:17Le 10:11; 26:46; Sl 119:5
Deut. 26:17De 13:18; Mla 12:13
Deut. 26:17Le 19:37; Sl 19:9
Deut. 26:17De 15:5
Deut. 26:18Eks 19:5; De 14:2; Sl 135:4
Deut. 26:18De 29:13
Deut. 26:19De 4:8; 28:1; Sl 148:14
Deut. 26:19De 7:6; 28:9
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 26:1-19

Deuteronomo

26 “Ndiyeno ukakalowa m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa monga cholowa chako, n’kulitenga kukhala lako ndi kukhalamo,+ 2 ukatenge zina mwa zipatso zoyambirira+ pa zipatso zonse za m’munda mwako zimene udzakolola m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa. Ukaziike m’dengu ndi kupita nazo kumalo amene Yehova Mulungu wako adzasankhe kuika dzina lake.+ 3 Uzikapita kwa wansembe+ amene azidzatumikira masiku amenewo ndi kumuuza kuti, ‘Ndikuvomereza lero pamaso pa Yehova Mulungu wako, kuti ndalowadi m’dziko limene Yehova analumbirira makolo athu kuti adzatipatsa.’+

4 “Wansembeyo azikalandira dengulo m’manja mwako ndi kuliika pafupi ndi guwa lansembe la Yehova Mulungu wako. 5 Pamenepo uzikanena pamaso pa Yehova Mulungu wako kuti, ‘Bambo anga anali Msiriya+ wotsala pang’ono kufa. Anapita ku Iguputo+ ndi anthu ochepa chabe+ a m’banja lake kukakhala kumeneko monga mlendo, koma anakhaladi mtundu waukulu ndi wamphamvu kumeneko.+ 6 Ndipo Aiguputo anayamba kutichitira zoipa, kutizunza ndi kutigwiritsa ntchito yowawa yaukapolo.+ 7 Pamenepo tinayamba kufuulira Yehova Mulungu wa makolo athu,+ ndipo Yehova anamva mawu athu+ ndi kuona nsautso yathu, mavuto athu ndi kuponderezedwa kwathu.+ 8 Pamapeto pake Yehova anatitulutsa mu Iguputo ndi dzanja lamphamvu+ ndi mkono wotambasula,+ zoopsa zazikulu,+ zizindikiro ndi zozizwitsa.+ 9 Ndiyeno anatibweretsa kumalo ano ndi kutipatsa dziko ili, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+ 10 Choncho ndabweretsa zipatso zoyambirira mwa zipatso za m’dziko limene Yehova anandipatsa.’+

“Pamenepo uzikaziika pamaso pa Yehova Mulungu wako ndi kugwada pamaso pa Yehova Mulungu wako.+ 11 Uzikasangalala+ chifukwa cha zabwino zonse zimene Yehova Mulungu wako wapatsa iwe ndi nyumba yako, zimene wapatsa iweyo komanso Mlevi ndi mlendo wokhala pakati panu.+

12 “Ukamaliza kusonkhanitsa chakhumi chonse+ cha zokolola zako m’chaka chachitatu,+ chaka chopereka chakhumi, uzikapereka chakhumicho kwa Mlevi, mlendo wokhala pakati panu, mwana wamasiye* ndi mkazi wamasiye. Amenewa azidzadya ndi kukhuta chakhumicho m’mizinda yanu.+ 13 Ukatero uzidzanena pamaso pa Yehova Mulungu wako kuti, ‘Ndachotsa chinthu chopatulika m’nyumba mwanga ndi kuchipereka kwa Mlevi, mlendo wokhala pakati pathu, mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye.+ Ndachita zimenezi mogwirizana ndi malamulo onse amene munandipatsa. Sindinaphwanye malamulo anu kapena kuwaiwala.+ 14 Sindinadyeko zina mwa zimenezi pa nyengo yanga yakulira, kapena kutengapo zina mwa zimenezi ndili wodetsedwa, kapena kupereka gawo lake chifukwa cha munthu wakufa. Ndamvera mawu a Yehova Mulungu wanga. Ndachita mogwirizana ndi zonse zimene munandilamula. 15 Yang’anani pansi kuchokera kumwamba, kumalo anu oyera okhalako,+ ndipo mudalitse anthu anu Aisiraeli+ ndi dziko limene mwatipatsa, dziko loyenda mkaka ndi uchi,+ monga mmene munalumbirira makolo athu.’+

16 “Lero Yehova Mulungu wanu akukulamulani kutsatira malangizo ndi zigamulo+ zimenezi. Motero muzisunga ndi kutsatira zimenezi ndi mtima wanu+ wonse ndi moyo wanu wonse.+ 17 Inu lero mwachititsa Yehova kunena kuti adzakhala Mulungu wanu mukamayenda m’njira zake ndi kusunga malangizo,+ malamulo+ ndi zigamulo zake+ ndiponso kumvera mawu ake.+ 18 Ndipo lero Yehova wakuchititsani kunena kuti mudzakhala anthu ake, chuma chapadera,+ monga mmene anakulonjezerani,+ ndiponso kuti mudzasunga malamulo ake onse, 19 ndi kuti adzakukwezani pamwamba pa mitundu ina yonse imene anapanga.+ Zimenezi zidzakudzetserani chitamando, mbiri yabwino ndi kukongola, mukapitiriza kukhala anthu oyera kwa Yehova Mulungu wanu,+ monga mmene anakulonjezerani.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena