Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 3:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mlandu umenewu ubwerere pamutu+ pa Yowabu ndi pa nyumba yonse ya bambo ake. M’nyumba ya Yowabu+ simudzasowa munthu wa nthenda yakukha kumaliseche+ ndiponso wakhate.+ Simudzasowanso mwamuna wogwira ndodo yowombera nsalu,+ wokanthidwa ndi lupanga kapena wosowa mkate!”+

  • 1 Mafumu 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Iweyo uchite zinthu monga mwa nzeru zako,+ ndipo usalole kuti imvi zake zitsikire ku Manda*+ mwamtendere.+

  • 1 Mafumu 2:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Kenako Benaya mwana wa Yehoyada anapita+ kuchihemako n’kukakantha Yowabu ndi kumupha,+ ndipo anaikidwa m’manda panyumba pake m’chipululu.

  • Salimo 28:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Muwabwezere mogwirizana ndi zochita zawo,+

      Mogwirizana ndi kuipa kwa zochita zawo.+

      Abwezereni mogwirizana ndi ntchito za manja awo.+

      Abwezereni zochita zawo.+

  • Salimo 62:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Komanso kukoma mtima kosatha ndi kwanu, inu Yehova,+

      Pakuti inu mumabwezera aliyense mogwirizana ndi ntchito zake.+

  • Agalatiya 6:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Musanyengedwe,+ Mulungu sapusitsika.+ Chilichonse chimene munthu wafesa, adzakololanso chomwecho.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena