Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 23:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Sara anamwalirira ku Kiriyati-ariba,+ kapena kuti ku Heburoni,+ m’dziko la Kanani.+ Pamenepo Abulahamu analowa muhema kukamulira Sara.

  • Numeri 13:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Atapita ku Negebu,+ anakafika ku Heburoni.+ Kumeneko anapezako Ahimani, Sesai ndi Talimai,+ mbadwa za Anaki.*+ Mzinda wa Heburoni+ unamangidwa zaka 7 mzinda wa Zowani+ wa ku Iguputo usanamangidwe.

  • Yoswa 14:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 N’chifukwa chake mzinda wa Heburoni uli cholowa cha Kalebe mwana wa Yefune Mkenizi, kufikira lero. Anam’patsa mzindawo chifukwa iye anatsatira Yehova Mulungu wa Isiraeli ndi mtima wake wonse.+

  • Yoswa 20:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Choncho anasankha mizinda ina kuti ikhale yopatulika. Mizinda yake inali Kedesi+ ku Galileya m’dera lamapiri la Nafitali, Sekemu+ m’dera lamapiri la Efuraimu, Kiriyati-ariba,+ kutanthauza Heburoni, m’dera lamapiri la Yuda.

  • Yoswa 21:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anawapatsa Kiriyati-ariba,+ kutanthauza Heburoni.+ (Ariba anali tate wa Anaki.)+ Mzindawu, pamodzi ndi malo ouzungulira odyetserako ziweto, unali m’dera lamapiri la Yuda.+

  • Yoswa 21:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Malo ozungulira mzindawo ndi midzi yake, anawapereka kwa Kalebe mwana wa Yefune kuti akhale ake.+

  • 1 Samueli 30:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 a ku Heburoni+ ndi kumalo onse kumene Davide anafikako pamodzi ndi amuna amene anali kuyenda naye.

  • 2 Samueli 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Patapita nthawi, mafuko onse a Isiraeli anapita kwa Davide+ ku Heburoni+ ndi kumuuza kuti: “Ife ndife fupa lanu ndi mnofu wanu.+

  • 1 Mafumu 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Davide analamulira Isiraeli zaka 40.+ Ku Heburoni+ analamulira zaka 7,+ ndipo ku Yerusalemu analamulira zaka 33.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena