Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 18
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 18:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 18:24; De 10:9; Yos 13:33
  • +Nu 18:8; Yos 13:14; 1Ak 9:13

Deuteronomo 18:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 18:20

Deuteronomo 18:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 23:19; Nu 18:12; De 26:10; 2Mb 31:4; Ne 12:44

Deuteronomo 18:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 28:1; Nu 3:10; De 10:8; 17:12

Deuteronomo 18:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 35:2
  • +De 12:5; 16:2; Sl 26:8

Deuteronomo 18:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mb 31:2

Deuteronomo 18:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 7:10; Lu 10:7; 1Ti 5:18

Deuteronomo 18:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 18:26; De 12:30

Deuteronomo 18:10

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu ake enieni, “kudutsitsa pamoto.”

  • *

    Onani mawu a m’munsi pa Le 19:26.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 18:21; De 12:31; 2Mf 16:3; 2Mb 28:3; Sl 106:37; Yer 19:5; 32:35
  • +2Mf 17:17; Mac 16:16
  • +Le 19:26; Mac 19:19
  • +Eze 21:21
  • +Eks 22:18

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 24

    Galamukani!,

    9/8/1993, tsa. 13

Deuteronomo 18:11

Mawu a M'munsi

  • *

    Mawu akuti ‘kulodza’ kapena ‘kuchisa’ amatanthauza kupweteka kapena kulepheretsa munthu kuchita chinachake mwa njira ya matsenga.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 47:9
  • +Le 20:27; 1Mb 10:13
  • +Le 19:31; 2Mb 33:6
  • +1Sa 28:3, 11; Yes 8:19; Aga 5:20

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo, article 67

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 24

    Galamukani!,

    6/2012, ptsa. 10-11

Deuteronomo 18:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 18:24; De 9:4

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 24

Deuteronomo 18:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Sa 22:24; Sl 37:18; Mt 5:48; 2Pe 3:14

Deuteronomo 18:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 19:26; 2Mf 21:2, 6
  • +Yos 13:22
  • +Sl 147:20; Mac 14:16

Deuteronomo 18:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 49:10; Nu 24:17; Lu 7:16; 24:19; Yoh 1:45; 6:14; Mac 3:22; 7:37

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

    Nsanja ya Olonda,

    4/15/2009, ptsa. 24-28

    Galamukani!,

    4/8/2004, ptsa. 28-29

Deuteronomo 18:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:17; De 9:10
  • +Eks 20:19

Deuteronomo 18:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:28

Deuteronomo 18:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 34:28; Nu 12:3; Mki 3:1; Mt 4:2; 11:29; Lu 24:27, 44; Yoh 5:46
  • +Yoh 8:28; 17:8
  • +Yoh 12:49; 15:15; Ahe 1:2

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

    Nsanja ya Olonda,

    4/15/2009, ptsa. 24-28

    2/15/2000, ptsa. 22-24

    11/15/1991, ptsa. 28-31

Deuteronomo 18:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 3:23

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

Deuteronomo 18:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 13:1; Yer 14:14; 28:11; Eze 13:6; Mt 7:15
  • +De 13:2; 1Mf 18:19; Yer 23:13
  • +De 13:5; Yer 27:15; Zek 13:3

Deuteronomo 18:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Yo 4:1

Deuteronomo 18:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 28:15
  • +Miy 29:25

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 18:1Nu 18:24; De 10:9; Yos 13:33
Deut. 18:1Nu 18:8; Yos 13:14; 1Ak 9:13
Deut. 18:2Nu 18:20
Deut. 18:4Eks 23:19; Nu 18:12; De 26:10; 2Mb 31:4; Ne 12:44
Deut. 18:5Eks 28:1; Nu 3:10; De 10:8; 17:12
Deut. 18:6Nu 35:2
Deut. 18:6De 12:5; 16:2; Sl 26:8
Deut. 18:72Mb 31:2
Deut. 18:8Le 7:10; Lu 10:7; 1Ti 5:18
Deut. 18:9Le 18:26; De 12:30
Deut. 18:10Le 18:21; De 12:31; 2Mf 16:3; 2Mb 28:3; Sl 106:37; Yer 19:5; 32:35
Deut. 18:102Mf 17:17; Mac 16:16
Deut. 18:10Le 19:26; Mac 19:19
Deut. 18:10Eze 21:21
Deut. 18:10Eks 22:18
Deut. 18:11Le 20:27; 1Mb 10:13
Deut. 18:11Le 19:31; 2Mb 33:6
Deut. 18:111Sa 28:3, 11; Yes 8:19; Aga 5:20
Deut. 18:11Yes 47:9
Deut. 18:12Le 18:24; De 9:4
Deut. 18:132Sa 22:24; Sl 37:18; Mt 5:48; 2Pe 3:14
Deut. 18:14Le 19:26; 2Mf 21:2, 6
Deut. 18:14Yos 13:22
Deut. 18:14Sl 147:20; Mac 14:16
Deut. 18:15Ge 49:10; Nu 24:17; Lu 7:16; 24:19; Yoh 1:45; 6:14; Mac 3:22; 7:37
Deut. 18:16Eks 19:17; De 9:10
Deut. 18:16Eks 20:19
Deut. 18:17De 5:28
Deut. 18:18Eks 34:28; Nu 12:3; Mki 3:1; Mt 4:2; 11:29; Lu 24:27, 44; Yoh 5:46
Deut. 18:18Yoh 8:28; 17:8
Deut. 18:18Yoh 12:49; 15:15; Ahe 1:2
Deut. 18:19Mac 3:23
Deut. 18:20De 13:1; Yer 14:14; 28:11; Eze 13:6; Mt 7:15
Deut. 18:20De 13:2; 1Mf 18:19; Yer 23:13
Deut. 18:20De 13:5; Yer 27:15; Zek 13:3
Deut. 18:211Yo 4:1
Deut. 18:22Yer 28:15
Deut. 18:22Miy 29:25
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 18:1-22

Deuteronomo

18 “Ansembe achilevi, kapena kuti fuko lonse la Levi,+ asakhale ndi gawo kapena cholowa pakati pa Isiraeli. Iwo azidya nsembe zotentha ndi moto zoperekedwa kwa Yehova. Azidya cholowa chake.+ 2 Choncho asalandire cholowa pakati pa abale awo. Yehova ndiye cholowa chawo,+ monga mmene anawauzira.

3 “Ndipo izi ndi zinthu zimene ansembe ayenera kulandira kuchokera kwa anthu. Amene akupereka nsembe ya ng’ombe kapena nkhosa, azipereka kwa wansembe mwendo wakutsogolo, nsagwada ndi chifu. 4 Uziperekanso gawo loyamba la mbewu zako, vinyo wako watsopano, mafuta ndi ubweya wa nkhosa wometedwa moyambirira.+ 5 Pakuti iye ndi amene Yehova Mulungu wako wam’sankha pakati pa mafuko anu onse, kuti iye pamodzi ndi ana ake aimirire ndi kutumikira m’dzina la Yehova nthawi zonse.+

6 “Ngati Mlevi watuluka mu umodzi mwa mizinda yonse ya Isiraeli, umene iye anakhalamo kwa kanthawi,+ ndiyeno wabwera pamalo amene Yehova adzasankhe, chifukwa chakuti mtima wake walakalaka kukatumikira pamalopo,+ 7 azitumikiranso m’dzina la Yehova Mulungu wake mofanana ndi abale ake onse Alevi, amene aimirira kumeneko pamaso pa Yehova.+ 8 Ngakhale kuti wapeza chuma atagulitsa katundu wa makolo ake, gawo la chakudya chake lizikhala lofanana ndi ansembe onse.+

9 “Ukakalowa m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa, usakaphunzire kuchita zinthu zonyansa zimene anthu a mitundu imeneyo akuchita.+ 10 Pakati panu pasapezeke munthu wotentha mwana wake pamoto,*+ wolosera,+ wochita zamatsenga,+ woombeza,*+ wanyanga,+ 11 kapena wolodza* ena,+ aliyense wofunsira kwa wolankhula ndi mizimu,+ wolosera zam’tsogolo+ kapena aliyense wofunsira kwa akufa.+ 12 Pakuti aliyense wochita zimenezi ndi wonyansa kwa Yehova. Ndipo chifukwa chakuti anthu a mitundu ina akuchita zimenezi, Yehova Mulungu wako akuwapitikitsa pamaso pako.+ 13 Ukhale wopanda cholakwa pamaso pa Yehova Mulungu wako.+

14 “Mitundu imene ukuilanda dziko inali kumvera anthu ochita zamatsenga+ ndi olosera.+ Koma iwe, Yehova Mulungu wako sanakulole kuchita zimenezi.+ 15 Yehova Mulungu wanu adzakupatsani mneneri ngati ine, kuchokera pakati panu, kuchokera pakati pa abale anu, ndipo inu mudzamvere mneneri ameneyo.+ 16 Adzakupatsani mneneri poyankha zonse zimene munapempha Yehova Mulungu wanu ku Horebe, tsiku limene munasonkhana kuphiri.+ Munapempha kuti, ‘Tiloleni tisamvenso mawu a Yehova Mulungu wathu, ndipo tisaonenso moto waukulu uwu, kuopera kuti tingafe.’+ 17 Pamenepo Yehova anandiuza kuti, ‘Mawu onse amene iwo anena ali bwino.+ 18 Ndidzawapatsa mneneri ngati iwe kuchokera pakati pa abale awo.+ Ndidzaika mawu anga m’kamwa mwake,+ ndipo adzawauza zonse zimene ndidzamulamula.+ 19 Pamenepo munthu amene sadzamvera mawu anga amene iye adzalankhule m’dzina langa, adzayankha mlandu kwa ine.+

20 “‘Koma mneneri amene adzadzikuza mwa kulankhula m’dzina langa mawu amene sindinamulamule kuti alankhule,+ kapena kulankhula m’dzina la milungu ina,+ mneneri ameneyo afe ndithu.+ 21 Mumtima mwako ukanena kuti: “Tidzadziwa bwanji kuti si Yehova amene walankhula mawuwo?”+ 22 Mneneri akalankhula m’dzina la Yehova, koma mawuwo sanachitike kapena kukwaniritsidwa, ndiye kuti si Yehova amene walankhula mawu amenewo.+ Mneneriyo walankhula mawu amenewo mwa iye yekha, modzikuza. Iwe usachite naye mantha.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena