Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • rs tsamba 439-445
  • Zosonyezera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zosonyezera
  • Kukambitsirana za m’Malemba
Kukambitsirana za m’Malemba
rs tsamba 439-445

Zosonyezera

Zosonyezera zimenezi sizikuphatikiza mbali iriyonse ya ndandanda ya nkhani yaikulu iriyonse. Kuti mupeze mfundo zina, tembenukirani ku mu(mi)tu wo(yo)yenelera m’masamba a mmbuyomu ndi kuŵerenga mitu yankhani yaing’ono.

Abrahamu, akazi ake, 385

Adamu ndi Hava, 25-27

anali anthu enieni, 25, 26, 106

chifukwa chake timavutika ndi zimene Adamu anachita, 223-225

dipo la mbadwa zawo, 123, 124 kodi anapita kumwamba?, 204

tchimo—kodi ndilo “kakonzedwe” ka Mulungu?, 27, 118

tchimo, mmene liliri lothekera, 358

ukwati, 384

Akazi, aminisitala, 29

Baibulo silimaŵasonyeza kukhala anthu apansi, 27-29

chophimba kumutu, 29, 30

mafuta osalalitsa khungu ndi majuwelo, 31

Akristu

mmene mungadziŵire owona, 89, 90, 167, 168, 287

ndiwo mboni za Yehova ndi za Yesu, 280

Akuda, themberero pa Kanani, 236, 237

Akufa, chiukiriro chawo, 80, 109-114, 379, 380

kulankhula nawo, 154, 155, 189, 190-192

kumene iwo ali, 152, 153

maholide owakumbukira, 244, 245

mkhalidwe wao, 144, 153, 344

sangathandize kapena kuvulaza amoyo, 188

ubatizo wao, 366, 367

Alefa ndi Omega, 399

“Amayi wa Mulungu,” Mariya, 256, 257

Aminisitala, akazi, 29

Ana, 10

ana a Mulungu, 237

kubadwa opunduka, 226

kupoperedwa mwazi, 317

lingaliro la Mulungu pa osabadwa, 211

pa Armagedo, 40, 41

ubatizo wa makanda, 364, 365

Ana Aamuna a Mulungu, 158, 237

Aneneri, kudziŵikitsa owona ndi onama, 32-35

Aneneri Onyenga, 32-37

kodi ndiwo Mboni za Yehova?, 36, 37

Armagedo, 9, 37-42

idziŵikitsidwa, 37, 38

kumene imenyedwera, 38, 39

opulumuka, 40

Atumwi, kukhululukira machimo, 219

Petro, “thanthwelo”?, 196-198

Ayuda, 42-47

chiŵerengero cha 144 000, 208, 209

kodi ndiwo anthu osankhidwa?, 42-44

kukanidwa kwa Yesu monga Mesiya, 425

kuwachitira umboni, 22, 23

Babulo, chisonkhezero chachipembedzo lerolino, 49, 50

kuulula, 219, 220

maloto, 247

milungu yautatu, 49

mtanda, 304, 305

mzinda wakale, 47, 49

openda nyenyezi, 50, 120, 121

Petro m’Babulo, 199

Babulo Wamkulu, akudziŵikitsidwa, 47-51

kuthaŵa kofulumira, 51

Baibulo, 10, 52-62

kudalirika kwa matembenuzidwe, 57, 58, 328

kuliŵerenga nokha nkosakwanira, 89, 93, 94

maumboni a kuuziridwa, 54, 55

Banja, 10, 388

Boma, 62-66

chifukwa chake ulamuliro waumunthu umalephera kukhutiritsa, 62-65

lingaliro la Akristu ku ladziko, 368, 369

Ufumu wa Mulungu, 64-66, 375, 376

Chaka Chatsopano, mapwando ake, 243

Chakudya, chochuluka mu Ufumuwo, 378

mnofu wanyama, 314

Chamba, 250, 253

Chikhululukiro

atumwi analolezedwa kukhululukira, 219

Chikhulupiriro, 67-70

chifukwa chake siyense amene ali nacho, 67, 68

chikhulupiriro chokha nchosakwanira, 70, 97

mmene chingapezedwere, 68, 69

Chikondi, cha Mulungu, kodi chikaswedwa ndi Armagedo?, 41

cha pa munthu mnzathu, 88

chizindikiro cha chipembedzo chowona, 90

kusoŵeka m’dziko, 11

kuzirala, 264

Chikumbutso, akudya, 72

deti, 73, 74

kuchuluka kwa nthaŵi za kuchitika, 73, 74, 283, 284

tanthauzo, 70, 71

zizindikiro, 71, 72

Chilamulo cha Mose, kuchotsedwa, 348, 349

mbali “zadzoma” ndi “zamakhalidwe,” 347, 348

Chilango, chilango chamuyaya?, 146-149

kodi nsautso ndizo chilango cha Mulungu?, 227, 228

pambuyo pa imfa?, 344

Chilekaniro, chaukwati, 385, 386

Chilengedwe, 74-78

kuchikhulupilira, m’gawo lasayansi, 74-76

kufanana mumpangidwe, 77

magwero a zipangizo, 77, 78

nthaŵi yophatikizidwa, 78

Chilengedwe chonse, magwero ake, 56

Chilimbikitso, 79-82

Chimwemwe, 11, 62, 63, 204, 205

Chinjoka, chinalankhula kwa Hava, 26

Chipanduko, 325

Chipembedzo, 83-94

Babulo Wamkulu, 47-52

chifukwa chake kuli zipembedzo zambiri motero, 83

chimene chimapatula Mboni za Yehova, 270-272

cholinganizidwiratu, 87-88

chipembedzo chimodzi chokha chowona, 93, 275

kodi m’zonse muli abwino? 84, 85, 92, 93

kuchoka m’chipembedzo chamakolo, 85, 86

kuloŵana chikhulupiliro, 86, 87

mmene mungadziŵire chowona, 89, 90

Chipulumutso, 94-99

Ayuda, 44

kodi chiri cha awo amene saali “obadwanso”?, 159

kodi mutapulumitsidwa kamodzi mwapulumutsidwa nthaŵi zonse?, 96

kodi ncha anthu onse?, 94-96

kodi ncha 144 000 okha?, 98

zofunika, 97, 123, 124, 430

Chisalungamo, 11, 81

Chisangalalo, kuchilondola, 248, 249, 325, 326

Chisautso chachikulu, opulumuka, 216, 267, 268

Chisinthiko, 99-106

“anthu onga anyani” ojambulidwa, 103

cholembedwa cha zokwiriridwa zakale, 101, 102

dongosolo loŵerengera zaka, 229, 230

kodi chinagwiritsiridwa ntchito ndi Mulungu?, 76, 77, 105, 106

kodi chiri chausayansi?, 99, 100

kusavomerezana pakati pa asayansi, 100

masinthidwe, 102

Chisoni, pa imfa ya wokondedwa, 155

Chisudzulo, 386, 387

Chisungiko, 12, 379

Chitaganya

mkhalidwe wa Mboni za Yehova kulinga ku kuwongolera, 278, 279

Chitsenderezo, mpumulo wanthaŵi zonse, 63, 64

Chiukiriro, 107-114

cha kumwamba, 109

cha padziko lapansi, 110-114

kusiyana ndi kudziveka thupi, 177, 178

thupi loukitsidwa la Yesu, 107-109, 431

Chiukiro, 64

Chiwawa, 326

Chiweruzo, chiukiriro cha, 111

Chiweruzo cholungama, 65, 379

Chizunzo, chifukwa chake Mboni zimazunzidwa, 265, 278

chilimbikitso cha kupilira, 80, 81

‘Chizunzo chamuyaya,’ 146-149

Choikidwiratu, 114-121, 156

kodi chimaikiratu “nthaŵi ya kufa”?, 114

kodi chinthu chirichonse chinadziŵidwiratu ndi kulinganizidwiratu ndi Mulungu?, 116-120

kodi chinthu chiri chonse “ndicho chifuniro cha Mulungu,”? 115, 116

Cholinganizidwiratu, Adamu, 118

Akristu, 119, 120

ndicho “chifuniro cha Mulungu,” 115, 116

Yakobo ndi Esau, 119

Yudase Iskariote, 119

(Wonaninso “Choikidwiratu.”)

Chophimba kumutu, chifukwa chake chiri chofunika, 29, 30

Chowonadi, chowonadi chenicheni, 60, 61, 136, 137

Chuma, kudziwonetsera, 326

moyo wolamuliridwa ndi kuchikhumba, 326

Dipo, 121-127

ana, 226

chifukwa chake liri lofunika, 122-124

kodi liri ndi chiyambukiro chotani panjira imene tikugwiritsira ntchito miyoyo yathu?, 127

mmene imfa ya Yesu inaliri yosiyana, 122

opindulawo, chifukwa chake, 124-126

Dziko, 128-131

kuphatikizidwa kwachipembedzo, 50, 202

kutembenuzidwa, 381, 382

kutetezeredwa ku mzimu wake, 323-327

mapeto ake, 128, 233, 234

mkhalidwe wa Akristu kulinga ku, 90, 130, 272, 374

opulumuka mapeto, 267, 268

tanthauzo la mikhalidwe, 53, 261-266

wolamulira, 128, 129, 355, 356

Dziko lapansi, 131-135, 271

dziko lapansi kukhalabe kosatha, 37, 38, 131-133

kukhalapo ndi moyo wamuyaya, 207, 208

mpangadwe wa planeti, 56

ngati anthu sakafa, kodi munthu aliyense adzakhala kuti?, 113, 114, 135

nzika zake—kodi zidzabwerera kuchokera kumwamba?, 134, 217

opulumukirapo, pambuyo pa chimariziro cha dziko, 215, 216, 267, 268

Paradaiso wamtsogolo, 336-342, 380

umboni wa chilengedwe, 75

Esau, kodi anaikidwiratu?, 119

Filosofi, 136-139

Fodya, 251-254

Gehena, 148, 149

Gulu, 139-143

kodi nlofunika?, 87, 88

mmene mungadziŵire lowoneka la Mulungu, 143

umboni wakuti Mulungu ali nalo, 139-142

Hade, 144, 146, 337

Helo, 144-151

amene amapitako, 145

‘chizunzo chamuyaya,’ m’Chivumbulutso, 147, 148

Gehena, 148, 149

munthu wachuma ndi Lazaro, 149, 150

Imfa, 13, 14, 151-157

chiyembekezo cha chiukiriro, 80, 109- 114, 379

imfa ya Yesu njosiyana, 122

kodi iri ndi nthaŵi yoikidwiratu?, 114, 156

kodi Mulungu analinganizanji?, 151, 156, 291, 292

kodi pali chilango pambuyo pake?, 146-150, 344

lingaliro la Ababulo, 49

malipoti a “moyo wina,” 153-155

miyambo ya kulira maliro, 155, 156

moyo, 144, 145, 297

ya Adamu, kuchotsedwa, 380

yochititsidwa ndi kusuta fodya, 252, 253

Isitala, 242, 243

Israyeli, kukwaniritsidwa kwa ulosi wa Baibulo, 45-47

wauzimu, 46, 47

Kaini, mkazi wake, 235

Kagulu kopanda mwambo, chifukwa chake Mboni siziri, 273

Kalankhula, kochititsidwa ndi kugwidwa ndi mzimu, 285

konyansa, 326

Khamu lalikulu, chiyembekezo cha padziko lapansi, 209

lipulumuka chisautso chachikulu, 216

King James Version, 61, 62

Krisimasi, 239-241

Kubadwanso, 157-161

chifukwa chake kuli kofunikira, 157, 158

ngati simuli wotero, kodi muli ndi mzimu woyera?, 159, 160

ngati simuli wotero, kodi ndinu wopulumutsidwa?, 159

Kubweranso kwa Kristu, 161-165

kukhalapo, 161, 162, 165

kosawoneka, 162-164

Kuchiritsa, 166-170

kozizwitsa—kodi kumachitidwa ndi mzimu wa Mulungu lerolino?, 166, 167 170

ngozi m’kukhulupirira mizimu, 169, 192, 193

Kuchitira umboni, 90, 265, 300

kaamba ka Yehova ndi Yesu, 280

kunyumba ndi nyumba, 277

Kudziimira, kodi pali ufulu weniweni popanda miyezo Yabaibulo?, 170-173

mikhalidwe yoti ipeŵedwe, 173, 174

Kudziveka Thupi Lanyama, 174-178

kodi umboni wake, m’Baibulo?, 175-177

malingaliro achilendo a kuzoloŵerana ndi anthu ndi malo, 174, 175

nkosiyana ndi chiyembekezo cha Baibulo, 177, 178

Kudziŵa pasadakhale: wonani

“Choikidwiratu.”

Kugonana, 171, 179-183

kugonana kwa aziŵalo zofanana, 180-183

kunja kwa ukwati, 180

lingaliro la Baibulo, 179, 180

Kugonana kwa aziŵalo zofanana, 180-183

Kuikidwa mwazi, ana, 317

kugwiritsiridwa ntchito kwa mwazi wa anthu, 315

zoloŵa mmalo, 316

Kuipa, 68, 183-187

chifukwa chake kwachuluka motere, 183, 184

chifukwa chake Mulungu wakulola, 184-187

chifukwa chake pambuyo pa kukhazikitsidwa kwa Ufumu, 233

kodi ndiwo umboni wakuti kulibe Mulungu?, 307, 308

nsautso, kodi ndicho chilango cha Mulungu?, 227, 228

wokuchititsa, 118, 183, 184

Kukhalapo, kwa Kristu, 161-165, 261-266

Kukhalapo musanabadwe, 203

“Kukhaliridwa pakati kopanda uchimo,” kwa Mariya, 257, 258

Kukoma mtima, 11

Kukondetsa zinthu zakuthupi, 171, 326

Kulambira, chilengedwe chonse chitagwirizanitsidwa, 377

anthu, 327

kugwiritsiridwa ntchito kwa zifanizo, 49, 259, 333, 434-438

mtanda, 305, 306

sikonse kovomerezedwa ndi Mulungu, 83, 84

Yesu, 429

Kulambira mizimu, 190-195

anamgoneka, 248, 249

kodi muli chivulazo chotani m’kufunsira kwa wolankhula ndi mizimu?, 192, 193

kodi nkotheka kulankhula ndi akufa?, 190-192

kupeza chimasuko ku chisonkhezero chake, 195

Kulinganizidwiratu, onani “Choikidwiratu.”

Kulira maliro, a akufa, 155

Kuloŵa Mmalo Kwautumwi, 196-203

kodi Petro anali ku Roma?, 199

“mfungulo za ufumu,” 198, 199

mzera wa kuloŵa mmalo, 200

Petro, kodi ndiye “thanthwelo”?, 196, 197

Kuloŵana chikhulupiliro, 86, 87

Kumizidwa, 364

Kumwamba, 203-210

amene amapitako, 203-206, 208, 209

chifukwa chake ena amapita kumwamba, 109, 210

chiŵerengero cha opita kumwamba, 208, 209

kodi awo otengeredwa kumwamba adzabwereranso kudziko lapansi?, 134, 217

‘kutsika kwa Ambuye kuchokera kumwamba,’ 214

kutengedwa m’thupi, 212-218

matupi a anthu kumwamba, 107-110, 214, 215, 431

pamene Akristu atengeredwa kumwamba, 212-217

paradaiso, 335, 337, 338

thupi la Mariya, 258

Kunyada, 325

Kupenda nyenyezi, 50, 120, 121, 240

Kupereŵera kwa chakudya, m’masiku otsiriza, 262, 263

Kupezedwa kwa nyumba, 12, 13, 65, 378

Kusakhoza kufa,

magwero a chiphunzitso cha Dziko Lachikristu, 298, 299

miyoyo ya anthu siiri yosakhoza kufa, 153, 188, 297

Kusayeruzika, m’masiku otsiriza, 264

Kusiyana kwa atsogoleri achipembedzo ndi anthu wamba, 50

Kusuta fodya, 251-254

Kutaya mimba, 210-212

Kutaya mtima, 79-82

Kutembenuka, Ayuda, 44, 45

ufumu sukayembekezera kutembenuzidwa kwa dziko, 381, 382

Kutengedwa m’Thupi, 212-218

Kuthiriridwa mwazi, kusala mwazi, 313-315, 317, 318

mankhwala oloŵa mmalo, 316

Kutsenderezeka, mpumulo wosatha, 63-65

Kuulula, 218-222

Kuunika kozungulira mutu, 333, 334

Kuuziridwa, umboni m’Baibulo, 54-57

Kuvutika, 11, 222-229

amene ali ndi thayo lake, 116, 222, 223

ana obadwa opunduka, 226

chifukwa chake Mulungu wakulola, 222-229

kodi ndiko kumene Mulungu analinganiza?, 292

kodi ndiko umboni wakuti kulibe Mulungu?, 307, 308

Kuŵerengera zaka

‘nthaŵi zoikidwiratu za amitundu,’ 231-233

Kuwombeza, maseŵero, 193, 194

Madeti, kuŵerengera 1914, 231-233

njira za asayansi zoŵerengera zaka, 229, 230

nyengo za Chigumula chisanakhale za anthu, 230, 231

Mafuko a anthu, 234-239

magwero a akuda, 236, 237

magwero ofanana, 25, 234

zifukwa za mikhalidweyo, 235, 236

Mafuta osalalitsa khungu, ogwiritsiridwa ntchito ndi akazi, 31

Maholide, Chaka Chatsopano, 243

Isitala, 242, 243

Krisimasi, 239-241

maholide amtundu, 246

okumbukira “mizimu ya akufa,” 244, 245

Tsiku la Amayi, 245

Tsiku la Valentine, 245

Majini, kodi ndiwo mfungulo ya chisinthiko?, 102

Majuwelo, ogwiritsiridwa ntchito ndi akazi, 31

Makanda, imfa ya, 152

kupunduka kobadwa nako, 226

ubatizo, 364, 365

Makolo akale, akufa, sangathe kuthandiza kapena kuvulaza, 188

kuŵakonda adakali amoyo, 189

mauthenga ochokera kwa akufa?, 153, 155, 189

Malamulo Khumi, anachotsedwa, 348, 349

Malodza abwino, 193, 194

Maloto, 246, 247

Mankhwala (Anamgoneka), chamba, 250, 251, 253

fodya, 251-253

kuwonjoka ku, 253, 254

malamulo amakhalidwe abwino Abaibulo, 248, 249, 251-253

ziyambukiro, 250-253

Mantha, owopa akufa, 188

owopa Yehova, 422, 423

masiku otsiriza, 264, 265

Maplaneti, kodi pali moyo pa enawo?, 294

Mariya (Amayi ŵa Yesu), 254-261

kodi anakhaliridwa pakati popanda uchimo?, 257, 258

kodi ndiye “Amayi ŵa Mulungu,” 256, 257

kodi thupi lake laumunthu liri kumwamba?, 258

kulambiridwa, 259, 260

kupemphera kwa Mariya, 258, 259

namwali, 255, 256, 260, 261

Maseŵero, oloŵetsamo kuwombeza, 193, 194

Masiku Otsiriza, 11, 261-270

chifukwa chake akhalako kwanthaŵi yaitali motero, 268

chiyambi, mu 1914, 266, 267

tsopano ali mkati, 261-266, 268, 269

Masinthidwe, chisinthiko, 102, 103

Matembenuzidwe, kudalirika kwa Baibulo, 57, 58, 328

pamene mamasuliridwe a Baibulo asiyana, 402, 403

Matenda, kuchiritsa kosatha, 79, 169, 170, 378

kuchiritsa mwachikhulupiliro, 166, 167, 170

Matsenga, 50

Mavesi, a Baibulo—chifukwa chake ena akuwonekera kukhala osoŵeka, 329

Mayanjano, oipa, 172

Mbendera, lingaliro Lachikristu, 372, 373

Mboni za Yehova, 270-280

chifukwa chake zimazunzidwa, 278

kodi ndizo chipembedzo cha ku America?, 272

kodi ndizo chipembedzo chowona chokha?, 275

kulungamitsa malingaliro, 35, 36, 277

mmene ntchito yawo imalipiliridwira, 273

sindizo aneneri onyenga, 36, 37

zikhulupiriro zimene zimazilekanitsa, 270-272

ziyambi, 274

Mbudha, kumchitira umboni, 21, 22

Mdyerekezi, 352-357

Mesiya, chifukwa chake Ayuda anakana Yesu, 425, 426

Mfungulo za Ufumu, 198, 199

Mhindu, kumchitira umboni, 22

Mikayeli, akudziŵikitsidwa, 432, 433

Mipatuko, 273, 274, 299, 300

Misa, kodi imapereka mpumulo ku miyoyo m’purigatoriyo?, 284

kuchuluka kwa nthaŵi za kuchitidwa, 283, 284

kusandulizidwa kukhala thupi lenileni ndi mwazi weniweni, 280-282

nsembe, 280-283

Mitala, 384, 385

Mitambo, “kudza m’mitambo” kwa Yesu, 163, 164, 214

‘kukwatulidwa m’mitambo,’ 212, 213

Mkazi, kodi angakhale woposa mmodzi?, 384, 385

mbali yake m’banja Lachikristu, 28, 29

Mliri, masiku otsiriza, 264

M’Malirime kulankhula, 284-289

kodi mphatsoyo idzapitirizabe kwautali wotani? 287, 288

kodi ndiwo umboni wakuti munthuyo ali ndi mzimu woyera?, 285, 286

Mngelo Wamkulu, Yesu Kristu, 432, 433

Moto, kodi dziko lapansi lidzawonongedwa ndi moto?, 132-134

kubatizidwa nawo, 367, 368

Moto wa helo, magwero a chiphunzitsocho, 150, 151

Moyo (Life), 289-294

chifuno, 11, 12, 53, 290, 291

chiyambukiro chimene dipo liyenera kukhala nacho pa wathu, 127

kusauchitira ulemu, 248, 251-253

kutaya mimba, 210-212

moyo wamuyaya, 11, 12, 72, 73, 122-124, 207, 208, 292, 293

pa maplaneti ena?, 294

Moyo (Soul), chimene uwo uli, 294, 296

chiukiriro, 107

imfa, 144, 297, 344

kusakhoza kufa—magwero a chiphunzitsocho, 154, 298, 299

kudziveka thupi, 174-179

ngwosiyana ndi mzimu, 297, 298

Mpatuko, 299-302

mkhalidwe kulinga kwa ampatuko, 301

zizindikiro zoŵadziŵira, 300, 301

Mphatso za mzimu, chifukwa chake zinaperekedwa, 169

Mpulumutsi, Yehova, 400

Yesu Kristu, 390, 391, 400, 433, 434

Msilamu, kumchitira umboni, 23, 24

Mtanda, imfa ya Yesu, 302, 303

kuulambira, 305, 306

magwero a wa Dziko Lachikristu, 304, 305

Mtendere, 12, 377

Mtengo, imfa ya Yesu, 302, 303

Mtsogolo, chifukwa chake simuyenera kutembenukira ku mizimu, 193,

chimene Baibulo limaneneratu za, 12 116, 117, 376-381, 389, 390

Mulungu, 10, 306-313

dzina lake—kumene limapezeka m’matembenuzidwe Abaibulo, 415-419

“Mulungu wowona yekha,” 311, 397, 398

munthu weniweni, 309

umboni wa kukhalako, 307, 308, 312, 313

wopanda chiyambi, 309, 310

Yesu monga mulungu, 311, 397, 398, 400, 403, 404, 426-428

(Wonaninso “Yehova.”)

Mwazi, 313-319

Mzimu, kudziŵa awo amene ali ndi mzimu woyera, 159, 160, 285-287, 320, 321, 323

mphamvu yogwira ntchito ya moyo

—chimene chimaichitikira pa imfa, 297, 298, 321-323

mphamvu yogwira ntchito ya Mulungu, 319, 320, 393, 394, 398

ubatizo, 366-368

Mzimu wadziko, mikhalidwe, 323-327

Mzimu woyera: wonani “Mzimu.”

Namwali, Mariya, 255, 256

Ndale zadziko, kuloŵetsedwamo kwachipembedzo, 50

mkhalidwe wa Akristu, 371, 372

New World Translation, 327-331

dzina la Yehova m’Malemba Achikristu Achigiriki, 329

mavesi owonekera kukhala osoŵeka, 329

mtundu wa matembenuzidwe, 327, 328

otembenuza, 328

1914, kukhazikitsidwa kwa Ufumu, 231-233

lingaliro la olemba mbiri yadziko, 266, 267

Njala, m’masiku otsiriza, 262, 268

Nkhondo, ya Armagedo, 37-42

lingaliro Lachikristu, 369-371

m’masiku otsiriza, 261, 262

mtendere pa nkhondo, 12, 377

mu Israyeli wakale, 370

Tchalitchi cha Katolika, 202, 203

ya nyukliya, 37, 38, 131, 132

Nsautso, kodi ndizo chilango chochokera kwa Mulungu?, 227, 228

Ntchito, zogwirizana ndi chikhulupiliro, 70, 97

Ntchito yolembedwa, Ufumu udzagaŵira, 12, 13, 65, 378

“Nthaŵi zoikidwiratu za amitundu” mmene zimaŵerengedwera, 231-233

Nyenyezi, kupenda nyenyezi, 50, 120, 121

nyenyezi inatsogolera openda nyenyezi kwa Herode, 240, 241

Nyimbo zautundu, lingaliro Lachikristu, 372, 373

Nzeru, yaumunthu, 137-139

yowona, 136

Obwebweta, mauthenga ochokera kwa akufa, 189, 191, 192

Ogwidwa ndi mzimu, 166, 167, 285, 286

Oyera mtima, 331-335

kodi ali opanda uchimo uliwonse?, 334

kupemphera kwa, 332, 333

kuunika kokweteza mutu, 333, 334

zifanizo ndi zinthu zakale zopatulika, 333, 435, 436

Paradaiso, 335-339

wa padziko lapansi, 336, 380, 381

wochita zoipa m’Paradaiso, 337-339

Pemphero, 339-342

kwa Mariya, 258, 259

kwa “oyera mtima,” 332, 333

mapemphero a amene Mulungu amamva, 339, 340

mapemphero a amene Mulungu samavomereza, 340, 341

nkhani zoyenelera, 341, 342

Petro, Apapa sindiwo oloŵa mmalo ake, 200

kodi anali ku Roma kapena ku Babulo?, 199

‘mfungulo za ufumu,’ 198, 199

“thanthwelo”?, 196, 197

Phompho, Satana kubindikiritsidwamo, 356, 357

Purigatoriyo, 343-345

magwero a chiphunzitsocho, 343

Misa ya okhalamo, 284

Sabata, 345-351

lamlungu ndi mlungu, kodi nla Akristu?, 345, 346

tanthauzo kwa Akristu, 349-351

Satana Mdyerekezi, akugubitsa anthu kumka ku Armagedo, 41, 42

ali ndi thayo la kuipa, 183, 184

anaponyedwa kuchokera kumwamba, 233, 356, 357

chifukwa chake waloledwa kukhalako, 354, 355

chiyambi, 354

kuponyedwa kuphompho, 356, 357

mulungu wa dongosolo lino, 355, 356

munthu wauzimu, 352, 354

ndiye wolamulira wadziko, 355, 356

Sauli, analankhula ndi “Samueli” kudzera mwa mkazi wobwebweta, 191

Sayansi, Baibulo liri patsogolo pa zotulukiridwa ndi asayansi, 56, 57

imakhulupilira chilengedwe, 74-76

imakhulupilira Mulungu, 307

malingaliro otsutsana onena za chisinthiko, 99, 100

Sheoli, 144, 146

Solomo, akazi, 384, 385

Tchimo, chikhululukiro, 219, 365, 366

chiyambukiro pa unansi ndi Mulungu, 361

kodi lerolino kuli tchimo?, 359, 360

kodi oyera mtima alibe?, 334

kuulula, 198, 199

kuyeretsedwa ku, 344, 345, 365, 366

la Adamu, kodi ndilo ‘kulinganiza’ kwa Mulungu? 27, 118

Mariya, kodi analibe tchimo?, 257, 258

mmene lirili lotheka kwa cholengedwa changwiro, 358, 359

ladala, 218, 219, 221, 222, 358

Thanthwe, Kristu, osati Petro, 196, 197

Themberero, fuko la akuda?, 236, 237

Thupi la munthu, linalinganizidwira kukhalako kosatha, 293

umboni wa chilengedwe, 75, 76

Tsiku, utali wa la kulenga, 78, 103, 104

Tsiku la Amayi, 245

Tsiku la kubadwa, 361-363

Tsiku la Valentine, 245

Ubatizo, kumizidwa m’madzi, 364-366

ndi moto, 367, 368

ndi mzimu woyera, 366-368

“wa akufa,” 366, 367

Uchete, 368-374

kuphatikizidwa m’ndale zadziko, 371, 372

mbendera ndi nyimbo zautundu, 372-374

nkhondo yazida, 369-371

Ufumu, 13, 374-382

boma, 375, 376

chimene udzakwaniritsa, 376-381

kuchitira umboni, 90, 265

“mfungulo za ufumu,” 198, 199

nthaŵi ya kukhazikitsidwa, 231-233, 381, 382

olamulira limodzi ndi Kristu, 157, 158, 208-210

Ukwati, chilekaniro, 385, 386

chisudzulo, 386, 387

kugonana usanachitike, 180

kulembetsedwa mwalamulo, 383, 384

mbale ndi mlongo, 387

mitala, 384, 385

mmene mungawongolere, 388

Ulamuliro, nkhaniyo, 184-186, 354, 355

ufumuwo umachirikiza wa Yehova, 376

Ulosi, 116, 118, 388-391

chifukwa chake muyenera kukhala wokondwerera kwambiri, 390, 391

kukwaniritsidwa, 54-56, 65, 66, 231-233 261-266

umene sunakwaniritsidwebe, 389, 390

Umbeta, 201, 202

Umodzi, wa chilengedwe chonse m’kulambira, 377

wa mafuko onse, 238, 239

Umutu, 28, 29

Upandu, 14

kuwonjezerekako kuli kwenikweni, 264

Utatu, 391-413

kodi malemba ogwiritsiridwa ntchito ndi okhulupilira utatu amapereka maziko olimba? 398-411

kodi malingaliro aakulu ophatikizidwa m’chiphunzitsochi ngogwirizana ndi Baibulo?, 393-398

magwero a chiphunzitsocho, 49, 200, 201, 392, 393

mkhalidwe wa owumamatira, 411, 412

Wachuma ndi Lazaro, fanizo, 149, 150

144 000, chiŵerengero chenicheni, 209

kodi ncha Ayuda akuthupi okha?, 208, 209

kodi ndiwo amene adzapulumuka okha?, 98, 99

Wochita zoipa, lonjezo la Paradaiso, 337, 339

Wokana Kristu, 414, 415

Yahweh, kodi ndiye Yehova kapena Yahweh?, 419, 420

Yakobo, akazi, 384, 385

kodi analinganizidwiratu?, 119

Yehova, 415-423

alibe chiyambi, 309, 310

dzinalo—kumene limapezeka m’Mabaibulo osiyanasiyana, 415-417

dzinalo m’Malemba Achikristu Achigiriki, 329, 418, 419

kodi ndilo dzina la Yesu mu “Chipangano Chakale”?, 421, 422

kodi ndiye Yahweh kapena Yehova?, 419, 420

kufunika kwa dzinalo, 420, 421

kuyeretsedwa kwa dzina lake, 376

Mulungu wowona yekha, 311, 397, 398, 400, 403, 404

(Wonaninso “Mulungu.”)

Yesu Kristu, 423-434

“Adamu wotsirizira,” 26, 123, 124

“akudza m’mitambo,” 163, 164, 214

anabadwa mwa namwali, 255

chifukwa chake Ayuda ambiri sanamlandire, 425, 426

chikumbutso cha imfa yake, 70-74, 282, 283

chiukiriro chathupi, 108, 109, 431, 432

imfa, 122

kodi imfa yake inali pamtengo kapena pamtanda?, 302, 303

kodi iye anali kokha munthu wabwino? 424

maina aulemu a Yehova anagwira ntchito kwa iye, 399, 400

Malemba Achihebri amene amalankhula za Yehova ndi amene anagwira ntchito kwa Yesu, 401

Mpulumutsi, 390, 391, 400, 430, 433, 434

waumulungu osati Mulungu, 403, 404, 426, 427

munthu weniweni, 423, 424

nsembe yadipo, 121-127, 314

“thanthwe,” 196

ufumu, 231-233, 381

umulungu, 413

‘woyamba wa chilengedwe,’ 394, 395

Yehova sindilo dzina lake, 421, 422

ziphunzitso zapamwamba, 138

zochitika zogwirizanitsidwa ndi kukhala pafupi kwake, 162, 165, 261-266

Yudase Iskariote, kodi analinganizidwiratu?, 119

Zakumwa zoledzeretsa

kusiyana kwake ndi chamba, 251

ziyambukiro pa omwererekera nazo, 171, 172

Zifanizo, 434-438

chifanizo kapena fano?, 434-436

kodi zimathandiza m’kulambira?, 435

Mariya, 259

Zachibabulo, 49

za “oyera mtima,” 333, 435, 436

Zigumukire, chifukwa chake Mulungu amalola “zachilengedwe,” 227

Zigumukire zachilengedwe (zotchedwa motero),

chifukwa chake zikuloledwa, 227

Zinyama, kukhetsa mwazi kaamba ka chakudya, 314

miyoyo, 295, 296

paubwenzi ndi anthu, 380

Zivomezi, chifukwa chake Mulungu akuzilola, 227

masiku otsiriza, 263, 268, 269

Ziŵanda, chisonkhezero pa mitundu, 41, 42, 63, 356

kodi zimatenga mpangidwe waumunthu?, 194

kulambira mizimu, 190-195, 352, 353

ziri ndi thayo la kuipa, 183, 184

Zizunzo, wachuma ndi Lazaro, 149, 150

zamuyaya m’Chivumbulutso, 147, 148

Zochiritsa, wonani “Kuchiritsa.”

Zokwiriridwa zakale, chisinthiko, 101, 102

Zosankha, kudalira pa kuŵerenga nyenyezi, 120, 121

kunyalanyaza chifuniro cha Mulungu, 172, 173, 324-327

Zozizwitsa, zamakono, 33, 166, 167

za Yesu, 378, 379, 429, 430

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena