Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • wcg tsamba 8-11
  • Zimene Zili M’bukuli

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Zili M’bukuli
  • Muziyenda Ndi Mulungu Molimba Mtima
  • Timitu
  • GAWO 1
  • Kuyambira Nthawi ya Inoki Kufika Nthawi ya Oweruza
  • GAWO 2
  • Kuyambira Nthawi ya Mafumu Kufika Nthawi Yomanganso Yerusalemu
  • GAWO 3
  • Nthawi ya Mesiya Komanso Otsatira Ake
Muziyenda Ndi Mulungu Molimba Mtima
wcg tsamba 8-11

Zimene Zili M’bukuli

Kalata Yochokera ku Bungwe Lolamulira 2

MAWU OYAMBA: Mukhoza Kukhala Olimba Mtima Kwambiri 4

GAWO 1

Kuyambira Nthawi ya Inoki Kufika Nthawi ya Oweruza

MUTU MUNTHU TSAMBA

Kuyambira Nthawi ya Inoki Kufika Nthawi ya Oweruza 12

Gawo 1 Nthawi Yomwe Zinthu Zinachitika 14

1 Anayenda Ndi Mulungu Inoki 16

2 Anatsutsa Dziko Nowa 20

3 Anakana Kumangoganizira Zam’mbuyo Sara 24

4 Munthu Woyamba Kumenya Nkhondo za Yehova Abulahamu 28

5 Anavomera Kuchita Chinthu Chovuta Kwambiri Abulahamu 32

6 Analolera Kusiya Achibale Ake Rabeka 36

7 Analimba Mtima Kuti Ateteze Banja Lake Yakobo 40

8 Sanagonje Atakumana Ndi Mayesero Yosefe 44

9 ‘Chifukwa cha Chikhulupiriro Anabisa Mose’ Sifira, Puwa, Amuramu, Yokebedi, Miriamu 48

10 Anasankha Zinthu Mwanzeru Mose 52

11 “Pita kwa Farao” Mose 58

12 Anakhalabe Wokhulupirika kwa Mulungu Wake Kalebe 62

13 Anatsatira Malangizo Achilendo Yoswa 66

14 Anasankha Yehova Kukhala Mulungu Wake Rahabi 70

15 Anathandizana pa Nthawi ya Mavuto Naomi ndi Rute 74

16 “Tipitiradi Limodzi” Baraki ndi Debora 78

17 “Mkazi Wodalitsika Kwambiri” Yaeli 82

18 Anali Wolimba Mtima Komanso Ankachita Zinthu Mosamala Gidiyoni 86

19 Anakwaniritsa Lumbiro Lovuta Yefita ndi Mwana Wake Wamkazi 90

20 Analimba Mtima pa Nthawi Yomwe Anali Wofooka Samisoni 94

21 Mnyamata Amene Analankhula Molimba Mtima Samueli 98

GAWO 2

Kuyambira Nthawi ya Mafumu Kufika Nthawi Yomanganso Yerusalemu

Kuyambira Nthawi ya Mafumu Kufika Nthawi Yomanganso Yerusalemu 102

Gawo 2 Nthawi Yomwe Zinthu Zinachitika 104

22 Anafunika Kulimba Mtima Kuti Akhalebe Wokhulupirika Yonatani 106

23 Analimba Mtima Kumenyana Ndi Chimphona Davide 110

24 Ankafunika Kulimbana Ndi Amuna Awiri Okwiya Abigayeli 114

25 Analimba Mtima Kuchita Zoyenera Davide 118

26 Anadzudzula Mfumu Natani 122

27 Sanakhumudwe Pamene Ankachitiridwa Zopanda Chilungamo Mefiboseti 126

28 Anatumikira Yehova Ndi Mtima Wonse “kwa Moyo Wake Wonse” Asa 130

29 “Mulungu Wanga Ndi Yehova” Eliya 134

30 Anasonyeza Kulimba Mtima pa Nthawi Yovuta Kwambiri Mayi Wamasiye wa ku Zarefati 138

31 Kamtsikana Kanalankhula Molimba Mtima Kudziko la Eni Kamtsikana ka ku Isiraeli 142

32 ‘Inu Yehova, Mutseguleni Maso’ Elisa 146

33 Anateteza Mfumu Yosankhidwa ndi Yehova Yehoyada 150

34 “Sanamusiye Yehova” Hezekiya 154

35 Analimba Mtima N’kulapa Manase 158

36 Anathandiza Anthu Kuti Ayambirenso Kulambira Yehova Yosiya 162

37 ‘Sanadzidetse’ Danieli 166

38 “Sanapse Ndi Moto” Aheberi Atatu 170

39 “Ngati Nʼkufa, Ndife” Esitere 176

40 Anamanganso Mpanda Nehemiya 180

GAWO 3

Nthawi ya Mesiya Komanso Otsatira Ake

Nthawi ya Mesiya Komanso Otsatira Ake 184

Gawo 3 Nthawi Yomwe Zinthu Zinachitika 186

41 “Anali Olungama Pamaso pa Mulungu” Zekariya ndi Elizabeti 188

42 Analimba Mtima N’kuvomera Mariya 192

43 Anali Bambo Wolimba Mtima Yosefe 196

44 ‘Palibe Wamkulu Kuposa Iyeyu’ Yohane M’batizi 200

45 “Ndine Munthu Wochimwa” Petulo 204

46 “Ambuye Ndawaona Ine!” Mariya wa ku Magadala 208

47 “Wachita Zimene Akanatha” Mariya, Mchemwali Wake wa Lazaro 212

48 “Munthu wa Chikhulupiriro Cholimba Ndiponso Wodzaza Ndi Mzimu Woyera” Sitefano 216

49 Anadzakhala Thanthwe Petulo 220

50 Anasintha Kwambiri Maganizo Ake Saulo wa ku Tariso 224

51 “Mwana Wotonthoza” Baranaba 228

52 “Amandithandiza” Maliko 232

53 “Musadandaule” Paulo 236

54 Analimba Mtima pa Nthawi Yovuta Mtumwi Yohane 242

MAWU OMALIZA: “Tikhale Olimba Mtima” 246

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena