Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 21
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Machitidwe 21:1

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 173-174

Machitidwe 21:2

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 173-174

Machitidwe 21:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 15:39
  • +Mac 20:3
  • +Mac 27:10

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 173-175

Machitidwe 21:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 21:11, 12

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, tsa. 175

Machitidwe 21:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eza 9:5; Mac 9:40; 20:36

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, tsa. 176

Machitidwe 21:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 18:21

Machitidwe 21:8

Mawu a M'munsi

  • *

    “Mlaliki” palembali akutanthauza “mmishonale.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 18:22
  • +Mac 6:5

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 176-177

    Nsanja ya Olonda,

    7/15/1999, tsa. 25

    9/1/1992, tsa. 17

Machitidwe 21:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yow 2:28; Mac 2:17; 1Ak 11:5

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 176-177

    Nsanja ya Olonda,

    7/15/1999, tsa. 25

    6/15/1990, tsa. 22

Machitidwe 21:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 11:28

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, tsa. 177

Machitidwe 21:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 20:23; 21:33
  • +Mac 9:16

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 177-178, 189

    Nsanja ya Olonda,

    6/15/1990, ptsa. 22-23

Machitidwe 21:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mt 16:22

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 177-178

Machitidwe 21:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 20:24
  • +De 20:8
  • +2Ak 4:10; 2Ti 4:6

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 177-178

    Nsanja ya Olonda,

    5/15/2008, tsa. 32

Machitidwe 21:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 3:18; Mt 26:42

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, tsa. 178

Machitidwe 21:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aro 15:25

Machitidwe 21:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 18:22

Machitidwe 21:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 24:11
  • +Mac 15:4

Machitidwe 21:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 12:17; 15:13; Aga 1:19; 2:9; Yak 1:1

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 112, 181

    Nsanja ya Olonda,

    5/15/1997, ptsa. 16-17

Machitidwe 21:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 11:4; 14:27
  • +Mac 15:12; Aro 15:18

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 181-182

Machitidwe 21:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 15:1; 22:3; Aro 10:2; Aga 1:14

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 182-183

    Nsanja ya Olonda,

    3/15/2003, ptsa. 23-24

    10/15/2002, tsa. 30

Machitidwe 21:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 6:14; Aga 5:1
  • +Aro 2:28; 1Ak 7:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 182, 183-185

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    9/2016, tsa. 15

    Nsanja ya Olonda,

    3/15/2003, tsa. 24

Machitidwe 21:23

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 184-185

    Nsanja ya Olonda,

    6/15/1990, tsa. 22

Machitidwe 21:24

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 6:2
  • +Nu 6:14, 15, 17
  • +Nu 6:18; Mac 18:18
  • +1Ak 9:20

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    10/2023, tsa. 10

    Kuchitira Umboni Mokwanira, ptsa. 184-185

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    10/2018, ptsa. 24-25

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    9/2016, tsa. 15

    Nsanja ya Olonda,

    3/15/2003, tsa. 24

    6/15/2000, tsa. 14

    6/15/1990, tsa. 22

    8/1/1987, ptsa. 12-14

Machitidwe 21:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 35:2; Eks 34:15; Mac 15:29
  • +Ge 9:4; Le 3:17; 17:10; De 12:23; 1Sa 14:32
  • +Le 17:13
  • +1Ak 6:9; Akl 3:5; 1At 4:3; 1Pe 4:3

Machitidwe 21:26

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 24:18; 1Ak 9:20
  • +Nu 6:5
  • +Nu 6:19, 21

Machitidwe 21:27

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 6:9
  • +Mac 19:29

Machitidwe 21:28

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 24:5
  • +Mac 24:6

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/2001, ptsa. 22-23

Machitidwe 21:29

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 20:4; 2Ti 4:20

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/2001, ptsa. 22-23

Machitidwe 21:30

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 17:5
  • +Mac 26:21

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    3/2020, tsa. 31

Machitidwe 21:31

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 21:27

Machitidwe 21:32

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 23:27
  • +Mac 23:26

Machitidwe 21:33

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 20:23; 21:11; Aef 6:20

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/2001, tsa. 21

    6/15/1990, ptsa. 22-23

Machitidwe 21:34

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 19:32
  • +Mac 22:24

Machitidwe 21:36

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Lu 23:18; Yoh 19:15; Mac 22:22

Machitidwe 21:37

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    2/15/2011, tsa. 5

Machitidwe 21:38

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 5:36

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    3/1/2010, tsa. 15

Machitidwe 21:39

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Afi 3:5
  • +Mac 9:11; 22:3

Machitidwe 21:40

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 13:16; 19:33
  • +Mac 26:14

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Mac. 21:3Mac 15:39
Mac. 21:3Mac 20:3
Mac. 21:3Mac 27:10
Mac. 21:4Mac 21:11, 12
Mac. 21:5Eza 9:5; Mac 9:40; 20:36
Mac. 21:6Mac 18:21
Mac. 21:8Mac 18:22
Mac. 21:8Mac 6:5
Mac. 21:9Yow 2:28; Mac 2:17; 1Ak 11:5
Mac. 21:10Mac 11:28
Mac. 21:11Mac 20:23; 21:33
Mac. 21:11Mac 9:16
Mac. 21:12Mt 16:22
Mac. 21:13Mac 20:24
Mac. 21:13De 20:8
Mac. 21:132Ak 4:10; 2Ti 4:6
Mac. 21:141Sa 3:18; Mt 26:42
Mac. 21:15Aro 15:25
Mac. 21:16Mac 18:22
Mac. 21:17Mac 24:11
Mac. 21:17Mac 15:4
Mac. 21:18Mac 12:17; 15:13; Aga 1:19; 2:9; Yak 1:1
Mac. 21:19Mac 11:4; 14:27
Mac. 21:19Mac 15:12; Aro 15:18
Mac. 21:20Mac 15:1; 22:3; Aro 10:2; Aga 1:14
Mac. 21:21Mac 6:14; Aga 5:1
Mac. 21:21Aro 2:28; 1Ak 7:19
Mac. 21:24Nu 6:2
Mac. 21:24Nu 6:14, 15, 17
Mac. 21:24Nu 6:18; Mac 18:18
Mac. 21:241Ak 9:20
Mac. 21:25Ge 35:2; Eks 34:15; Mac 15:29
Mac. 21:25Ge 9:4; Le 3:17; 17:10; De 12:23; 1Sa 14:32
Mac. 21:25Le 17:13
Mac. 21:251Ak 6:9; Akl 3:5; 1At 4:3; 1Pe 4:3
Mac. 21:26Mac 24:18; 1Ak 9:20
Mac. 21:26Nu 6:5
Mac. 21:26Nu 6:19, 21
Mac. 21:27Nu 6:9
Mac. 21:27Mac 19:29
Mac. 21:28Mac 24:5
Mac. 21:28Mac 24:6
Mac. 21:29Mac 20:4; 2Ti 4:20
Mac. 21:30Mac 17:5
Mac. 21:30Mac 26:21
Mac. 21:31Mac 21:27
Mac. 21:32Mac 23:27
Mac. 21:32Mac 23:26
Mac. 21:33Mac 20:23; 21:11; Aef 6:20
Mac. 21:34Mac 19:32
Mac. 21:34Mac 22:24
Mac. 21:36Lu 23:18; Yoh 19:15; Mac 22:22
Mac. 21:38Mac 5:36
Mac. 21:39Afi 3:5
Mac. 21:39Mac 9:11; 22:3
Mac. 21:40Mac 13:16; 19:33
Mac. 21:40Mac 26:14
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
  • 26
  • 27
  • 28
  • 29
  • 30
  • 31
  • 32
  • 33
  • 34
  • 35
  • 36
  • 37
  • 38
  • 39
  • 40
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Machitidwe 21:1-40

Machitidwe

21 Tsopano titadzikakamiza kulekana nawo n’kuyamba ulendo wathu wa panyanja, tinayenda molunjika mpaka kufika ku Ko. Koma tsiku lotsatira tinafika ku Rode, ndipo titachoka kumeneko tinakafika ku Patara. 2 Kumeneko tinapeza ngalawa imene inali kuwolokera ku Foinike, ndipo tinakwera ndi kunyamuka. 3 Chilumba cha Kupuro+ chitayamba kuonekera, tinachisiya kumanzere ndi kupitiriza ulendo wathu kulowera ku Siriya.+ Tinaima ku Turo, chifukwa kumeneko ngalawa inafunika kutsitsa katundu.+ 4 Titafufuza tinapeza ophunzira ndi kukhala nawo kumeneko masiku 7. Koma mouziridwa ndi mzimu,+ iwo anauza Paulo mobwerezabwereza kuti asakaponde mu Yerusalemu. 5 Choncho titatsiriza masikuwo, tinanyamuka kuti tipitirize ulendo wathu. Ndipo abale onse, pamodzi ndi amayi ndi ana, anatiperekeza mpaka kunja kwa mzindawo. Kumeneko tinagwada+ pagombe ndi kupemphera 6 n’kutsanzikana.+ Kenako ife tinakwera ngalawa ndipo iwo anabwerera kunyumba zawo.

7 Choncho tinanyamuka ku Turo pangalawa ndipo tinafika ku Tolemayi. Kumeneko tinalonjerana ndi abale ndi kukhala nawo tsiku limodzi. 8 M’mawa mwake tinanyamuka ndi kukafika ku Kaisareya.+ Kumeneko tinakalowa m’nyumba ya mlaliki* Filipo. Iyeyu anali mmodzi wa amuna 7 a mbiri yabwino aja,+ ndipo tinakhala naye. 9 Mwamuna ameneyu anali ndi ana aakazi anayi, anamwali, amene anali kunenera.+ 10 Koma titakhala masiku ndithu, mneneri wina dzina lake Agabo+ anafika kumeneko kuchokera ku Yudeya. 11 Iye anafika kwa ife ndi kutenga lamba wa Paulo. Kenako anadzimanga mapazi ndi manja ndi kunena kuti: “Mzimu woyera wati, ‘Mwiniwake wa lambayu, Ayuda adzamumanga+ chonchi ku Yerusalemu ndi kumupereka+ m’manja mwa anthu a mitundu ina.’” 12 Titamva zimenezi, ife pamodzi ndi anthu akumeneko, tinayamba kuchonderera Paulo kuti asapite+ ku Yerusalemu. 13 Koma Paulo anayankha kuti: “N’chifukwa chiyani mukulira+ ndi kunditayitsa mtima?+ Dziwani kuti ine ndine wokonzeka osati kumangidwa kokha, komanso kukafa+ ku Yerusalemu chifukwa cha dzina la Ambuye Yesu.” 14 Titalephera kumusintha maganizo, tinangovomereza ndi kunena kuti: “Chifuniro+ cha Yehova chichitike.”

15 Masiku amenewa atapita, tinakonzekera ulendo ndipo tinanyamuka kulowera ku Yerusalemu.+ 16 Koma ophunzira ena a ku Kaisareya+ ananyamuka nafe, kuti atiperekeze kunyumba ya munthu wina kuti tikafikire kumeneko. Munthu ameneyu dzina lake linali Mnaso wa ku Kupuro, ndipo anali mmodzi wa ophunzira oyambirira. 17 Titafika ku Yerusalemu,+ abale anatilandira mokondwa.+ 18 Koma tsiku lotsatira, Paulo anapita nafe kwa Yakobo,+ ndipo akulu onse anali komweko. 19 Paulo anawalonjera ndi kuyamba kuwafotokozera mwatsatanetsatane+ zimene Mulungu anachita pakati pa anthu a mitundu ina kudzera mu utumiki wake.+

20 Iwo atamva zimenezi anayamba kutamanda Mulungu, ndipo anamuuza kuti: “M’bale, kodi ukuona kuchuluka kwa okhulupirira amene ali pakati pa Ayuda? Ndipo onsewa ndi odzipereka pa nkhani yotsatira Chilamulo.+ 21 Komatu iwo amva mphekesera zakuti iwe wakhala ukuphunzitsa Ayuda onse amene ali pakati pa anthu a mitundu ina kuti apandukire Chilamulo cha Mose.+ Akuti ukuwauza kuti asamachite mdulidwe+ wa ana awo kapena kutsatira miyambo imene takhala tikuitsatira kuyambira kale. 22 Tsopano tichite chiyani pamenepa? Sitikukayikira kuti iwo adzamva ndithu kuti iwe wafika. 23 Choncho uchite zimene tikuuze pano: Tili ndi amuna anayi amene anachita lumbiro. 24 Utenge amuna amenewa+ ndipo ukachite mwambo wa kudziyeretsa pamodzi ndi iwo. Uwalipirire zonse zofunika,+ kuti amete tsitsi lawo.+ Ukatero, aliyense adzadziwa kuti mphekesera zimene anamva za iwe ndi nkhambakamwa chabe. Adzaona kuti ukuchita zinthu motsatira dongosolo, komanso kuti umasunga Chilamulo.+ 25 Koma kwa okhulupirira ochokera mwa anthu a mitundu inawo, tinawatumizira chigamulo chathu chakuti apewe zoperekedwa nsembe kwa mafano+ komanso magazi,+ zopotola,+ ndi dama.”+

26 Choncho Paulo anatenga amunawo tsiku lotsatira ndi kukachita mwambo wa kudziyeretsa pamodzi ndi iwo.+ Kenako analowa m’kachisi, kukanena pamene masiku awo a mwambo wa kudziyeretsa adzathere,+ ndi pamene aliyense wa iwo adzamuperekere nsembe.+

27 Ali pafupi kutsiriza masiku 7,+ Ayuda ochokera ku Asia anaona Paulo ali m’kachisi. Chotero anayambitsa chisokonezo+ m’khamu lonse la anthu ndipo anamugwira. 28 Iwo anali kufuula kuti: “Inu Aisiraeli, tithandizeni! Munthu amene akuphunzitsa zotsutsana ndi anthu a mtundu wathu kulikonse ndi ameneyu.+ Iyeyu akuphunzitsa zotsutsana ndi Chilamulo komanso malo ano. Kuwonjezera pamenepo, inu mukudziwa kuti anatenga Agiriki n’kudzawalowetsa m’kachisi ndipo waipitsa malo oyera ano.”+ 29 Iwo ananena zimenezi chifukwa tsiku lina anaona Terofimo+ wa ku Efeso ali naye limodzi mumzindawo. Atawaona anaganiza kuti Paulo analowetsa Terofimo m’kachisi. 30 Chotero munali chisokonezo mumzinda wonsewo, ndipo anthu anali balalabalala+ kuthamangira kukachisiko. Kenako anagwira Paulo ndi kumukokera kunja kwa kachisi.+ Nthawi yomweyo zitseko zinatsekedwa. 31 Ndipo pamene anali kufuna kumupha, uthenga unafika kwa mtsogoleri wa gulu la asilikali kuti mu Yerusalemu monse muli chisokonezo.+ 32 Mwamsanga, iye anatenga asilikali ndi akapitawo awo ndi kuthamangira kumeneko.+ Anthuwo ataona mkulu wa asilikali+ uja pamodzi ndi asilikali akewo, analeka kumenya Paulo.

33 Pamenepo mkulu wa asilikali uja anafika pafupi ndi kumugwira ndipo analamula kuti amumange ndi maunyolo awiri.+ Ndiyeno anafunsa za iye kuti anali ndani ndiponso zimene anachita. 34 Koma ena m’khamulo anayamba kufuula zinthu zina, enanso zina.+ Choncho, atalephera kutolapo mfundo yeniyeni chifukwa cha phokoso, analamula kuti apite naye kumpanda wa asilikali.+ 35 Ndiyeno atafika pamasitepe, asilikaliwo anachita kumunyamula chifukwa chakuti khamulo linali kuchita chiwawa. 36 Khamu la anthu linali kuwatsatira, likufuula kuti: “Aphedwe ameneyo!”+

37 Koma atatsala pang’ono kulowa naye kumpanda wa asilikali, Paulo anauza mkulu wa asilikali kuti: “Mungandilole kodi kulankhula nanu pang’ono?” Iye anati: “Kodi umalankhula Chigiriki? 38 Kodi si iwe Mwiguputo uja amene masiku apitawo unayambitsa chipolowe choukira boma+ ndi kutsogolera zigawenga 4,000 kupita nazo m’chipululu?” 39 Pamenepo Paulo ananena kuti: “Inetu ndine Myuda+ wa ku Tariso,+ ku Kilikiya, nzika ya mzinda wotchuka. Chonde ndikukupemphani, kuti mundilole ndilankhule kwa anthuwa.” 40 Atamulola, Paulo anaimirira pamasitepe ndi kukwezera anthuwo dzanja.+ Onse atakhala phee, analankhula nawo m’Chiheberi,+ kuti:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena