Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Deuteronomo 28:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 15:26; Le 26:3; Yes 1:19; Lu 1:6
  • +De 26:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/1995, ptsa. 26-27

Deuteronomo 28:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Miy 10:22

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/2010, ptsa. 19-20

    9/15/2010, tsa. 8

    9/15/2001, tsa. 10

Deuteronomo 28:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 107:36
  • +De 11:14

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/15/1996, tsa. 15

Deuteronomo 28:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:9; De 7:13; Sl 127:3; 128:3
  • +De 30:9
  • +Sl 107:38

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/15/1996, ptsa. 15-16

Deuteronomo 28:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 26:2
  • +Eks 12:34; 23:25; Ru 1:6

Deuteronomo 28:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 27:17; De 31:2; 2Mb 1:10; Sl 91:14; 121:8

Deuteronomo 28:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:7; De 32:30; Yos 10:11; 2Sa 22:38; Sl 89:23
  • +De 7:23; 2Mb 14:13; Ahe 11:34

Deuteronomo 28:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:10; Miy 3:10; Mki 3:10
  • +De 15:10

Deuteronomo 28:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 7:6; 1Pe 1:15
  • +Ge 17:7; Eks 19:6; De 7:8; Ahe 6:13
  • +De 27:1

Deuteronomo 28:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Nu 6:27; 2Mb 7:14; Yes 43:10; 63:19; Da 9:19; Mac 15:17
  • +Nu 22:3; De 11:25; Yos 5:1

Deuteronomo 28:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:4
  • +De 30:9; Sl 65:9
  • +Ge 15:18

Deuteronomo 28:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:4; De 11:14; Yer 14:22
  • +De 14:29; 15:10; Sl 67:7; 115:13
  • +De 15:6

Deuteronomo 28:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Mf 4:21
  • +Sl 119:98

Deuteronomo 28:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:32; Yos 1:7; Miy 4:27; Yes 30:21
  • +Le 19:4; De 11:16; Sl 96:5; 1Ak 8:4

Deuteronomo 28:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:16; Da 9:11; Mki 2:2; Aga 3:13

Deuteronomo 28:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 7:12; 26:6; Mlr 1:1
  • +1Mf 17:1; Yow 1:4; Hag 1:6

Deuteronomo 28:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 26:2
  • +Le 26:26; Mik 6:14

Deuteronomo 28:18

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 5:9; Mlr 2:11, 19; 4:10; Ho 9:12
  • +Le 26:20
  • +Le 26:22

Deuteronomo 28:19

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mb 15:5

Deuteronomo 28:20

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mki 2:2
  • +1Sa 4:10; 2Mf 14:12
  • +Sl 39:11; 80:16; Yes 30:17; 51:20; Eze 5:15
  • +Le 26:31; De 4:26; Yos 23:16

Deuteronomo 28:21

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:25; Yer 21:6; 24:10

Deuteronomo 28:22

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:16
  • +Le 26:33; Yer 16:4
  • +1Mf 8:37
  • +2Mb 6:28; Amo 4:9; Hag 2:17

Deuteronomo 28:23

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:19; De 11:17; 1Mf 8:35; 17:1; Yer 14:4; Amo 4:7

Deuteronomo 28:25

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:17; De 32:30
  • +Yer 24:9; 29:18; Eze 23:46; Lu 21:24

Deuteronomo 28:26

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Sa 17:44; Sl 79:2; Yer 7:33

Deuteronomo 28:27

Mawu a M'munsi

  • *

    Ena amati “matenda a mdidi,” kapena “matenda otuluka thumbo.”

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 7:15; Amo 4:10

Deuteronomo 28:28

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mla 7:7
  • +Eks 4:11; Le 26:16
  • +Yer 4:9

Deuteronomo 28:29

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 59:10; Zef 1:17
  • +Owe 3:14; 6:4; Ne 9:27; Sl 106:42

Deuteronomo 28:30

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 8:10
  • +Yes 5:9; Mlr 5:2; Zef 1:13
  • +Amo 5:11; Mik 6:15

Deuteronomo 28:31

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Sa 22:42

Deuteronomo 28:32

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mb 29:9; Yow 3:6
  • +Ne 5:5

Deuteronomo 28:33

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:16; De 28:51; Ne 9:37; Yes 1:7; Yer 5:17
  • +Zek 11:6

Deuteronomo 28:34

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:67

Deuteronomo 28:35

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:27; Yob 2:7

Deuteronomo 28:36

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mf 17:6; 25:26; Yes 39:7
  • +2Mf 25:7; 2Mb 33:11; 36:6; Yer 22:11
  • +De 4:28; Yer 16:13

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Ulosi wa Danieli, ptsa. 71-72

Deuteronomo 28:37

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Mf 9:8; Yer 25:9
  • +2Mb 7:20; Sl 44:14; Yer 24:9

Deuteronomo 28:38

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 5:10; Hag 1:6
  • +1Mf 8:37; 2Mb 6:28; Yow 2:3, 25

Deuteronomo 28:39

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Zef 1:13
  • +Yon 4:7

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    6/15/2006, tsa. 18

Deuteronomo 28:40

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mik 6:15

Deuteronomo 28:41

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:32; 2Mf 24:14; Yer 52:15, 30; Mlr 1:5

Deuteronomo 28:43

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 25:47

Deuteronomo 28:44

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 15:5, 6; Miy 22:7
  • +Eza 9:7

Deuteronomo 28:45

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:15; 29:27; Yer 26:6
  • +Le 26:28; 2Mf 17:20; Yes 1:20; Yer 24:10
  • +De 11:28; Sl 119:21; Yer 7:24

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/1995, ptsa. 15-16

Deuteronomo 28:46

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 25:18; Eze 14:8; 1Ak 10:11

Deuteronomo 28:47

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ne 8:10; Sl 100:2
  • +De 12:7; 32:15; Ne 9:35

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/1995, ptsa. 15-16

Deuteronomo 28:48

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mb 12:8; Yer 5:19; 17:4
  • +Yer 44:27
  • +Yer 28:14

Deuteronomo 28:49

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yer 6:22; Hab 1:6
  • +Yes 28:11; Yer 5:15
  • +Yer 4:13; Mlr 4:19; Ho 8:1

Deuteronomo 28:50

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eze 21:31
  • +2Mb 36:17; Yes 47:6; Lu 19:44

Deuteronomo 28:51

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:33
  • +Le 26:26; Yer 15:13

Deuteronomo 28:52

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +2Mf 17:5; 25:1; Yer 39:1; Lu 19:43

Deuteronomo 28:53

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:29; 2Mf 6:28; Yer 19:9; Mlr 2:20; 4:10; Eze 5:10

Deuteronomo 28:54

Mawu a M'munsi

  • *

    Munthu wosasatitsidwa ndi munthu wopusa chifukwa chakuti anamulera momulekerera ndipo sanaphunzire ntchito kapena zinthu zina zomuthandiza pamoyo wake.

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 15:9; Miy 23:6

Deuteronomo 28:55

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:48; Yer 52:6

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    8/1/1989, tsa. 29

Deuteronomo 28:56

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mlr 4:5

Deuteronomo 28:57

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 49:15
  • +De 28:53

Deuteronomo 28:58

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 24:7; Le 26:15; De 31:26
  • +Eks 14:4; Le 10:3; Sl 72:19
  • +De 10:17; Ne 1:5; Sl 99:3; Yes 29:23
  • +Eks 3:15; 6:3; 20:2; Sl 83:18; 113:3; Yes 42:8; Mki 2:2

Deuteronomo 28:59

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:21; 2Mb 21:14; Da 9:12
  • +De 28:22; 2Mb 21:15

Deuteronomo 28:60

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 7:12, 15; 28:27; Amo 4:10

Deuteronomo 28:62

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 10:22; 26:5; Ne 9:23
  • +De 4:27

Deuteronomo 28:63

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 30:9
  • +Miy 1:26
  • +Yer 12:14; 18:7

Deuteronomo 28:64

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Le 26:33; De 4:27; Ne 1:8; Lu 21:24
  • +De 4:28; 28:36; Yer 16:13

Deuteronomo 28:65

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eze 5:12; Amo 9:4
  • +Le 26:36; Eze 12:19
  • +Le 26:16

Deuteronomo 28:66

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ahe 10:27

Deuteronomo 28:67

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +De 28:34

Deuteronomo 28:68

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 14:13; Yer 44:12; Ho 9:3
  • +Ne 5:8

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Deut. 28:1Eks 15:26; Le 26:3; Yes 1:19; Lu 1:6
Deut. 28:1De 26:19
Deut. 28:2Miy 10:22
Deut. 28:3Sl 107:36
Deut. 28:3De 11:14
Deut. 28:4Le 26:9; De 7:13; Sl 127:3; 128:3
Deut. 28:4De 30:9
Deut. 28:4Sl 107:38
Deut. 28:5De 26:2
Deut. 28:5Eks 12:34; 23:25; Ru 1:6
Deut. 28:6Nu 27:17; De 31:2; 2Mb 1:10; Sl 91:14; 121:8
Deut. 28:7Le 26:7; De 32:30; Yos 10:11; 2Sa 22:38; Sl 89:23
Deut. 28:7De 7:23; 2Mb 14:13; Ahe 11:34
Deut. 28:8Le 26:10; Miy 3:10; Mki 3:10
Deut. 28:8De 15:10
Deut. 28:9De 7:6; 1Pe 1:15
Deut. 28:9Ge 17:7; Eks 19:6; De 7:8; Ahe 6:13
Deut. 28:9De 27:1
Deut. 28:10Nu 6:27; 2Mb 7:14; Yes 43:10; 63:19; Da 9:19; Mac 15:17
Deut. 28:10Nu 22:3; De 11:25; Yos 5:1
Deut. 28:11De 28:4
Deut. 28:11De 30:9; Sl 65:9
Deut. 28:11Ge 15:18
Deut. 28:12Le 26:4; De 11:14; Yer 14:22
Deut. 28:12De 14:29; 15:10; Sl 67:7; 115:13
Deut. 28:12De 15:6
Deut. 28:131Mf 4:21
Deut. 28:13Sl 119:98
Deut. 28:14De 5:32; Yos 1:7; Miy 4:27; Yes 30:21
Deut. 28:14Le 19:4; De 11:16; Sl 96:5; 1Ak 8:4
Deut. 28:15Le 26:16; Da 9:11; Mki 2:2; Aga 3:13
Deut. 28:16Yer 7:12; 26:6; Mlr 1:1
Deut. 28:161Mf 17:1; Yow 1:4; Hag 1:6
Deut. 28:17De 26:2
Deut. 28:17Le 26:26; Mik 6:14
Deut. 28:18De 5:9; Mlr 2:11, 19; 4:10; Ho 9:12
Deut. 28:18Le 26:20
Deut. 28:18Le 26:22
Deut. 28:192Mb 15:5
Deut. 28:20Mki 2:2
Deut. 28:201Sa 4:10; 2Mf 14:12
Deut. 28:20Sl 39:11; 80:16; Yes 30:17; 51:20; Eze 5:15
Deut. 28:20Le 26:31; De 4:26; Yos 23:16
Deut. 28:21Le 26:25; Yer 21:6; 24:10
Deut. 28:22Le 26:16
Deut. 28:22Le 26:33; Yer 16:4
Deut. 28:221Mf 8:37
Deut. 28:222Mb 6:28; Amo 4:9; Hag 2:17
Deut. 28:23Le 26:19; De 11:17; 1Mf 8:35; 17:1; Yer 14:4; Amo 4:7
Deut. 28:25Le 26:17; De 32:30
Deut. 28:25Yer 24:9; 29:18; Eze 23:46; Lu 21:24
Deut. 28:261Sa 17:44; Sl 79:2; Yer 7:33
Deut. 28:27De 7:15; Amo 4:10
Deut. 28:28Mla 7:7
Deut. 28:28Eks 4:11; Le 26:16
Deut. 28:28Yer 4:9
Deut. 28:29Yes 59:10; Zef 1:17
Deut. 28:29Owe 3:14; 6:4; Ne 9:27; Sl 106:42
Deut. 28:30Yer 8:10
Deut. 28:30Yes 5:9; Mlr 5:2; Zef 1:13
Deut. 28:30Amo 5:11; Mik 6:15
Deut. 28:312Sa 22:42
Deut. 28:322Mb 29:9; Yow 3:6
Deut. 28:32Ne 5:5
Deut. 28:33Le 26:16; De 28:51; Ne 9:37; Yes 1:7; Yer 5:17
Deut. 28:33Zek 11:6
Deut. 28:34De 28:67
Deut. 28:35De 28:27; Yob 2:7
Deut. 28:362Mf 17:6; 25:26; Yes 39:7
Deut. 28:362Mf 25:7; 2Mb 33:11; 36:6; Yer 22:11
Deut. 28:36De 4:28; Yer 16:13
Deut. 28:371Mf 9:8; Yer 25:9
Deut. 28:372Mb 7:20; Sl 44:14; Yer 24:9
Deut. 28:38Yes 5:10; Hag 1:6
Deut. 28:381Mf 8:37; 2Mb 6:28; Yow 2:3, 25
Deut. 28:39Zef 1:13
Deut. 28:39Yon 4:7
Deut. 28:40Mik 6:15
Deut. 28:41De 28:32; 2Mf 24:14; Yer 52:15, 30; Mlr 1:5
Deut. 28:43Le 25:47
Deut. 28:44De 15:5, 6; Miy 22:7
Deut. 28:44Eza 9:7
Deut. 28:45De 28:15; 29:27; Yer 26:6
Deut. 28:45Le 26:28; 2Mf 17:20; Yes 1:20; Yer 24:10
Deut. 28:45De 11:28; Sl 119:21; Yer 7:24
Deut. 28:46Yer 25:18; Eze 14:8; 1Ak 10:11
Deut. 28:47Ne 8:10; Sl 100:2
Deut. 28:47De 12:7; 32:15; Ne 9:35
Deut. 28:482Mb 12:8; Yer 5:19; 17:4
Deut. 28:48Yer 44:27
Deut. 28:48Yer 28:14
Deut. 28:49Yer 6:22; Hab 1:6
Deut. 28:49Yes 28:11; Yer 5:15
Deut. 28:49Yer 4:13; Mlr 4:19; Ho 8:1
Deut. 28:50Eze 21:31
Deut. 28:502Mb 36:17; Yes 47:6; Lu 19:44
Deut. 28:51De 28:33
Deut. 28:51Le 26:26; Yer 15:13
Deut. 28:522Mf 17:5; 25:1; Yer 39:1; Lu 19:43
Deut. 28:53Le 26:29; 2Mf 6:28; Yer 19:9; Mlr 2:20; 4:10; Eze 5:10
Deut. 28:54De 15:9; Miy 23:6
Deut. 28:55De 28:48; Yer 52:6
Deut. 28:56Mlr 4:5
Deut. 28:57Yes 49:15
Deut. 28:57De 28:53
Deut. 28:58Eks 24:7; Le 26:15; De 31:26
Deut. 28:58Eks 14:4; Le 10:3; Sl 72:19
Deut. 28:58De 10:17; Ne 1:5; Sl 99:3; Yes 29:23
Deut. 28:58Eks 3:15; 6:3; 20:2; Sl 83:18; 113:3; Yes 42:8; Mki 2:2
Deut. 28:59Le 26:21; 2Mb 21:14; Da 9:12
Deut. 28:59De 28:22; 2Mb 21:15
Deut. 28:60De 7:12, 15; 28:27; Amo 4:10
Deut. 28:62De 10:22; 26:5; Ne 9:23
Deut. 28:62De 4:27
Deut. 28:63De 30:9
Deut. 28:63Miy 1:26
Deut. 28:63Yer 12:14; 18:7
Deut. 28:64Le 26:33; De 4:27; Ne 1:8; Lu 21:24
Deut. 28:64De 4:28; 28:36; Yer 16:13
Deut. 28:65Eze 5:12; Amo 9:4
Deut. 28:65Le 26:36; Eze 12:19
Deut. 28:65Le 26:16
Deut. 28:66Ahe 10:27
Deut. 28:67De 28:34
Deut. 28:68Eks 14:13; Yer 44:12; Ho 9:3
Deut. 28:68Ne 5:8
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
  • 18
  • 19
  • 20
  • 21
  • 22
  • 23
  • 24
  • 25
  • 26
  • 27
  • 28
  • 29
  • 30
  • 31
  • 32
  • 33
  • 34
  • 35
  • 36
  • 37
  • 38
  • 39
  • 40
  • 41
  • 42
  • 43
  • 44
  • 45
  • 46
  • 47
  • 48
  • 49
  • 50
  • 51
  • 52
  • 53
  • 54
  • 55
  • 56
  • 57
  • 58
  • 59
  • 60
  • 61
  • 62
  • 63
  • 64
  • 65
  • 66
  • 67
  • 68
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Deuteronomo 28:1-68

Deuteronomo

28 “Ukamveradi mawu a Yehova Mulungu wako mwa kuonetsetsa kuti ukutsatira malamulo ake onse amene ndikukupatsa lero,+ Yehova Mulungu wako adzakukweza ndithu pamwamba pa mitundu yonse ya padziko lapansi.+ 2 Madalitso onsewa adzakutsata ndi kukupeza+ chifukwa ukumvera mawu a Yehova Mulungu wako:

3 “Udzakhala wodalitsika mumzinda,+ udzakhala wodalitsika m’munda.+

4 “Chidzadalitsika chipatso cha mimba yako,+ chipatso cha m’dziko lanu, chipatso cha ziweto zako,+ ana a ng’ombe zako ndi ana a nkhosa zako.+

5 “Lidzadalitsika dengu lako+ ndi chiwiya chako chokandiramo ufa.+

6 “Udzadalitsika pa zochita zako zonse.+

7 “Yehova adzachititsa adani ako amene adzakuukira kugonja pamaso pako.+ Pobwera kwa iwe adzadutsa njira imodzi, koma pothawa pamaso pako, adzadutsa njira 7.+ 8 Yehova adzaika madalitso pankhokwe+ ndi pa zochita zako zonse+ ndipo adzakudalitsa m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa. 9 Yehova adzakukhazikitsani monga anthu ake oyera,+ monga mmene analumbirira kwa inu,+ chifukwa mwapitiriza kusunga malamulo+ a Yehova Mulungu wanu ndipo mwayenda m’njira zake. 10 Pamenepo mitundu yonse ya anthu padziko lapansi adzaona kuti mukutchedwa ndi dzina la Yehova,+ ndipo adzachita nanu mantha.+

11 “Yehova adzachulukitsa chuma chako pa zipatso za mimba yako,+ zipatso za ziweto zako ndi zipatso za m’munda mwako,+ m’dziko limene Yehova analumbirira makolo ako kuti adzakupatsa.+ 12 Yehova adzakutsegulira kumwamba, nyumba yake yabwino yosungiramo zinthu, kuti akupatse mvula pa nyengo yake+ m’dziko lako ndi kuti adalitse ntchito iliyonse ya manja ako.+ Udzakongoza mitundu yambiri koma iwe sudzakongola kanthu kwa iwo.+ 13 Yehova adzakuchititsa kukhala kumutu osati kumchira. Pamenepo udzangokhala pamwamba+ ndipo sudzakhala m’munsi, chifukwa ukumvera malamulo+ a Yehova Mulungu wako amene ndikukupatsa lero kuti uwasunge ndi kuwatsatira. 14 Usapatuke pa mawu onse amene ndikukulamula lero, kupita kudzanja lamanja kapena lamanzere+ kuti utsatire milungu ina ndi kuitumikira.+

15 “Mukapanda kumvera mawu a Yehova Mulungu wanu ndi kuonetsetsa kuti mukutsatira malamulo ake onse ndi mfundo zake zimene ndikukupatsani lero, matemberero otsatirawa adzakugwerani ndi kukupezani:+

16 “Udzakhala wotembereredwa mumzinda,+ udzakhala wotembereredwa m’munda.+

17 “Lidzakhala lotembereredwa dengu lako+ ndi chiwiya chako chokandiramo ufa.+

18 “Chidzakhala chotembereredwa chipatso cha mimba yako,+ chipatso cha nthaka yako,+ ana a ng’ombe zako ndi ana a nkhosa zako.+

19 “Udzakhala wotembereredwa pa zochita zako zonse.+

20 “Yehova adzakutumizira matemberero,+ chisokonezo+ ndi chilango+ pa ntchito zako zonse zimene ukuyesa kugwira. Adzakuchitira zimenezi kufikira utafafanizidwa ndi kutha mofulumira, chifukwa cha kuipa kwa zochita zako popeza kuti wandisiya.+ 21 Yehova adzachititsa mliri kukumamatira kufikira atakufafaniza m’dziko limene ukupita kukalitenga kukhala lako.+ 22 Yehova adzakulanga ndi chifuwa chachikulu,+ kuphwanya kwa thupi koopsa, kutupa, kutentha thupi kwambiri, lupanga,+ mphepo yotentha yowononga mbewu+ ndi matenda a mbewu.+ Zimenezi zidzakusautsa kufikira utawonongeka. 23 Thambo limene lili pamwamba pa mutu wako lidzakhala ngati mkuwa, ndipo nthaka yako idzakhala ngati chitsulo.+ 24 Yehova adzakugwetsera mchenga ndi fumbi ngati mvula m’dziko lako. Adzakugwetsera zimenezi kuchokera kumwamba kufikira utafafanizika. 25 Yehova adzakuchititsani kuti mugonje pamaso pa adani anu.+ Pokamenyana nawo nkhondo mudzadutsa njira imodzi, koma pothawa pamaso pawo mudzadutsa njira 7. Mudzakhala chinthu chonyansa kwa mafumu onse a dziko lapansi.+ 26 Mitembo yanu idzakhala chakudya cha cholengedwa chilichonse chouluka m’mlengalenga ndi zilombo zakutchire, ndipo sipadzakhala woziopsa.+

27 “Yehova adzakulanga ndi zithupsa za ku Iguputo,+ matenda a mudzi,* ziwengo ndi zotupa, ndipo sudzachira matenda amenewa. 28 Yehova adzakulanga ndi misala,+ khungu+ ndipo adzakuchititsa kudabwa kwambiri.+ 29 Udzafufuzafufuza masana ngati mmene wakhungu amafufuzirafufuzira mu mdima,+ ndipo sudzapambana. Iwe wekha udzakhala wodyeredwa ndi kulandidwa zinthu nthawi zonse, popanda wokupulumutsa.+ 30 Udzalonjeza kukwatira mkazi koma mwamuna wina adzamugwirira.+ Udzamanga nyumba koma sudzakhalamo.+ Udzabzala mitengo ya mpesa koma sudzadya zipatso zake.+ 31 Ng’ombe yako idzaphedwa iwe ukuona, koma nyama yake sudzadyako. Bulu wako adzalandidwa ndi achifwamba iwe ukuona, ndipo sudzamuonanso. Nkhosa yako idzaperekedwa kwa adani ako, koma sipadzakhala wokupulumutsa.+ 32 Ana ako aamuna ndi ana ako aakazi adzaperekedwa kwa anthu ena+ iwe ukuona ndipo udzawalakalaka nthawi zonse, koma manja ako adzakhala opanda mphamvu.+ 33 Anthu amene sunawadziwe adzadya zipatso za m’dziko lako ndi mbewu zako zonse.+ Motero udzakhala wodyeredwa ndi woponderezedwa nthawi zonse.+ 34 Pamenepo udzasokonezeka mutu chifukwa cha zimene maso ako adzaona.+

35 “Yehova adzakulanga ndi zithupsa zonyeka m’mawondo onse ndi m’ntchafu monse. Matenda amenewa adzayambira kumapazi mpaka paliwombo, ndipo sudzachira.+ 36 Yehova adzakuyendetsa+ pamodzi ndi mfumu+ yako imene udzadziikira, kukupititsa ku mtundu umene iweyo kapena makolo ako simunaudziwe. Kumeneko udzatumikira milungu ina, yamtengo kapena yamwala.+ 37 Pamenepo udzakhala chodabwitsa,+ adzakupekera mwambi+ ndi kukutonza pakati pa mitundu yonse ya anthu amene Yehova adzakupititsako.

38 “Udzapita ndi mbewu zambiri kumunda, koma udzakolola zochepa+ chifukwa dzombe lidzadya mbewuzo.+ 39 Udzalimadi ndi kubzala mitengo ya mpesa, koma sudzakolola mphesa zake ndi kumwa vinyo,+ chifukwa mbozi zidzadya mpesawo.+ 40 Udzakhala ndi mitengo ya maolivi m’dera lako lonse, koma sudzadzola mafuta chifukwa maolivi ako adzayoyoka.+ 41 Udzabereka ana aamuna ndi ana aakazi, koma sadzapitiriza kukhala ako chifukwa adzatengedwa kupita ku ukapolo.+ 42 Mitengo yako yonse ndi zipatso za m’dziko lako zidzakhala za tizilombo ta mapiko tochita mkokomo. 43 Mlendo wokhala pakati panu adzapitirizabe kutukuka kukuposani, koma inuyo mudzapitirizabe kutsika pansi.+ 44 Iye adzakhala wokukongoza koma iweyo sudzatha kumukongoza.+ Iye adzakhala mutu koma iweyo udzakhala mchira.+

45 “Matemberero onsewa+ adzakugwera, kukutsatira ndi kukupeza kufikira utafafanizika,+ chifukwa sunamvere mawu a Yehova Mulungu wako mwa kusunga malamulo ndi mfundo zake zimene anakupatsa.+ 46 Matembererowa adzapitiriza pa iwe ndi ana ako monga chizindikiro ndi cholosera mpaka kalekale,+ 47 chifukwa chakuti sunatumikire Yehova Mulungu wako mokondwera, ndi mtima wosangalala,+ pamene unakhala ndi zochuluka pa chilichonse.+ 48 Udzatumikira adani ako+ amene Yehova adzawatuma kuti akuukire. Udzawatumikira uli ndi njala,+ ludzu, usiwa ndiponso ukusowa china chilichonse. Adzakuveka goli lachitsulo m’khosi lako kufikira atakufafaniza.+

49 “Yehova adzautsa mtundu wakutali, kumalekezero a dziko,+ mtundu umene chilankhulo chake sudzachimva.+ Mtunduwo udzakuukira monga mmene chiwombankhanga chimakhwathulira nyama yake,+ 50 mtundu wa nkhope yoopsa+ umene sudzaikira kumbuyo munthu wachikulire kapena kukondera mnyamata.+ 51 Iwo adzadya chipatso cha ziweto zako ndi zipatso za nthaka yako kufikira utafafanizidwa,+ ndipo sadzakusiyirako mbewu, vinyo watsopano kapena mafuta, mwana wa ng’ombe yako kapena mwana wa nkhosa yako kufikira atakuwonongeratu.+ 52 Chotero adzakuzungulirani m’mizinda yanu yonse kufikira mipanda yanu yaitali ndi yolimba kwambiri imene muzidzaidalira itagwa m’dziko lanu lonse. Adzakuzungulirani ndithu m’mizinda yanu yonse m’dziko lanu limene Yehova Mulungu wanu wakupatsani.+ 53 Pamenepo udzadya chipatso cha mimba yako, mnofu wa ana ako aamuna ndi ana ako aakazi,+ amene Yehova Mulungu wako wakupatsa, chifukwa cha zovuta ndi nsautso zimene adani ako adzakupanikiza nazo.

54 “Koma mwamuna wolobodoka nkhongono ndi wachisasati* pakati panu, adzayang’ana ndi diso+ loipa m’bale wake, mkazi wake wokondedwa ndi ana ake aamuna amene atsala, 55 kuti asagawireko aliyense wa iwo mnofu uliwonse wa ana ake aamuna amene adzawadya. Adzatero poona kuti alibiretu china chilichonse, chifukwa cha zovuta ndi nsautso zimene mdani wanu adzakupanikizani nazo m’mizinda yanu yonse.+ 56 Ndipo mkazi wolobodoka nkhongono ndi wachisasati pakati panu, amene sanayesepo n’komwe kupondetsa phazi lake pansi chifukwa cha kuleredwa mwachisasati ndi kulobodoka nkhongono,+ ameneyu adzayang’ana ndi diso loipa mwamuna wake wokondedwa, mwana wake wamwamuna ndi mwana wake wamkazi. 57 Adzayang’ananso ndi diso loipa zotuluka m’mimba mwake pambuyo pobereka komanso ana ake aamuna amene iye anabereka,+ chifukwa adzawadya mseri pokhala wosowa chilichonse chifukwa cha zovuta ndi nsautso zimene mdani wanu adzakupanikizani nazo m’mizinda yanu.+

58 “Ngati sudzatsatira mosamala mawu onse a chilamulo ichi olembedwa m’buku ili,+ kuti uziopa dzina laulemerero+ ndi lochititsa manthali,+ dzina lakuti Yehova,+ amene ndi Mulungu wako, 59 Yehova adzakulitsa kwambiri miliri yako ndi miliri ya ana ako. Miliri imeneyo idzakhala yaikulu kwambiri ndi yokhalitsa,+ ndipo udzagwidwa ndi matenda onyansa ndi okhalitsa.+ 60 Adzakubweretsera matenda onse a ku Iguputo amene unachita nawo mantha, ndipo adzakumamatira.+ 61 Kuwonjezera pamenepo, Yehova adzakubweretsera nthenda iliyonse ndi mliri uliwonse umene sunalembedwe m’buku la chilamulo ili, kufikira utafafanizika. 62 Ngakhale kuti mwachuluka ngati nyenyezi zakumwamba,+ mudzatsala ochepa+ chifukwa chosamvera mawu a Yehova Mulungu wanu.

63 “Chotero, monga mmene Yehova anasangalalira kuti akuchitireni zabwino ndi kukuchulukitsani,+ momwemonso adzasangalala kuti akuwonongeni ndi kukufafanizani.+ Pamenepo mudzatheratu m’dziko limene mukupita kukalitenga kukhala lanu.+

64 “Yehova adzakumwazani mwa anthu a mitundu yonse kuchokera kumalekezero ena a dziko mpaka kumalekezero enanso a dziko.+ Kumeneko mukatumikira milungu ina imene inuyo kapena makolo anu simunaidziwe, milungu yamtengo ndi milungu yamwala.+ 65 Pakati pa mitundu imeneyo sudzakhala mwamtendere,+ ndipo sudzapeza malo oti phazi lako liponde kuti lipumulirepo. Kumeneko, Yehova adzakupatsa mtima wachinthenthe,+ adzachititsa maso ako+ khungu ndipo adzakutayitsa mtima. 66 Pamenepo moyo wako udzakhala pangozi yaikulu koopsa, ndipo udzakhala wamantha usiku ndi usana, moti sudzakhala wotsimikiza za moyo wako.+ 67 M’mawa udzanena kuti, ‘Zikanakhala bwino akanakhala madzulo!’ ndipo madzulo udzanena kuti, ‘Zikanakhala bwino ukanakhala m’mawa!’ chifukwa cha mantha amene adzagwira mtima wako, ndiponso chifukwa cha zimene maso ako adzaona.+ 68 Yehova adzakubwezerani ku Iguputo pa zombo kudzera njira imene ndinakuuzani kuti, ‘Simudzaionanso.’+ Kumeneko mudzalakalaka kudzigulitsa kwa adani anu kuti mukhale akapolo aamuna ndi aakazi,+ koma sipadzakhala wokugulani.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena